Search

LIVRES NUMÉRIQUES ET LIVRES AUDIO GRATUITS

La Première Epître de Jean

Chichewa  14

Paul C. Jong’s Kukula Mumzimu Mundandanda wa 3 - Kalata Woyamba Wa Yohane (Ⅰ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239269 | Pages 337

Téléchargez des livres numériques et livres audio GRATUITS

Choisissez votre format de fichier préféré et téléchargez-le en toute sécurité sur votre appareil mobile, PC ou tablette pour lire et écouter les collections de sermons n'importe quand et n'importe où. Tous les livres numériques et livres audio sont entièrement gratuits.

Vous pouvez écouter le livre audio via le lecteur ci-dessous. 🔻
Possédez un livre broché
Téléchargement gratuit de livres audio
Zamakati
 
Kalambulabwalo

CHAPITALA 1
1. Yesu Khristu Ndi Mulungu (1 Yohane 1:1-10) 
2. Kodi Mulidi pa Mugwirizano ndi Mulungu? (1 Yohane 1:1-10) 
3. Mitundu Iwiri ya Kumvomereza (1 Yohane 1:8-10) 
4. Kuvomereza mu Choonadi (1 Yohane 1:8-10) 

CHAPITALA 2
1. Yesu Khristu Ndi Mulungu Woona (1 Yohane 2:1-5) 
2. Ambuye Athu Amene Anakhala Mthandizi Wathu (1 Yohane 2:1-17) 
3. Kodi Inu M’kukhala mu Lamulo La Mulungu? (1 John 2:7-11) 
4. Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za Mdziko (1 Yohane 2:15-17) 
5. Kodi Adani a Khristu Ndani (1 Yohane 2:18-29) 
 
Mtumwi Yohane ndi mumodzi wa atsogoleri aakulu mumzimu mu Chikhristu. Makalata onse atatu iye analemba akuchitilabe umboni wa wa Choonadi wa cha poyera ndi mumzimu ku woyera mu Mpingo wa Mulungu. Koma muli ndime zina zimene ndi zikosa kuti ife timasulire ndi kumvetsa.
Tingapereke 1Yohane 1:8 ngati chisanzo cha ndime zobvuta mu Makalata ya Yohane: Tikanena kuti: “Tilibe uchimo,” ndiye kuti tikudzinamiza ndipo mwa ife mulibe choonadi.” Ndimeyi ndiyobvuta kumvetsa, maka-maka ngati taigwiritsa nchito ku okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu.
Chisanzo chachiwiri ndi 1 Yohane 1:9, “Mulungu ndiwokhulupirika ndiponso wolungama, chotero tikavomereza machimo athu, adzatikhululukira ndi kutiyeretsa ku ntchito zonse zoipa.” Iyi yakhala ndime yakunenedwa pafupipafupi ngati ochimwa akufuna kupereka mfundo zabaibulo za mapemphero awo akulapa. Ndiyeno, ndimeyi ikutanthauza kuti ochimwa afunika kuvomereza machimo awo kuti akhululukidwe kumachimo awo amene anachita kodi? Kapena, kodi chikutanthauza kuti olungama amene okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu ayenera kuvomereza machimo awo? Tifunika kukhulupilira ndimeyi malinga ndi kamsulidwe ka Mzimu Woyera, Mlembi wa Baibulo, ndiponso kumalingaliro a Mtumwi Yohane.
Chisanzo cha chitatu cha ndime yobvuta ndi 1 Yohane 2:22, “Kodi wabodza angakhalenso ndani, kuposa amene amatsutsa kuti Yesu ndiye Khristu? Ameneyu ndiye wokana Khristu, amene amakana Atate ndi Mwana.” Ndimeyi ikulankhula za amene ndi adani a Mulungu. Ndimeyi ikufotokoza poyera kuti adani a Mulungu ndi onse aja sakhulupilira kuti Yesu ndi Mulungu. Ndipo ichi chikutanthauzanso kuti sakuthokoza Atate a Yesu Khristu ngati Mulungu.
Chachinayi ndi 1 Yohane 3:6 imene ikuti, “Yense wakukhala mwa Iye sachimwa yense wakuchimwa sanamuone Iye, ndipo sanamdziwe Iye.” Apa, ngati taona mawu, yense wakukhala mwa iye,” ndimeyi akuperekedwa ku olungama amene anayeretsedwa kumachimo awo onse mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Olungama sangakane chikhulupiliro chawo muzokhoma zilizonse cifukwa akukhulupilira mu uthenga woona. Kodi kungakhaledi ena amene sakuchita machimo ndi mathupi awo? Aliyense akuchita uchimo. Koma, okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu sangachite uchimo otero ngati wakukana uthenga woona.
Plus

Livres liés à ce titre

The New Life Mission

Participez à notre enquête

Comment avez-vous entendu parler de nous ?