Search

BUKU ELEKTRONIK DAN BUKU AUDIO GRATIS

Bidah

Chichewa  25

Ampatuko, Amene Anasatira Machimo a YEROBOWAMU (I)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928241774 | Halaman 332

Unduh buku elektronik dan buku audio GRATIS

Pilih format file yang Anda inginkan dan unduh dengan aman ke perangkat seluler, PC, atau tablet Anda untuk membaca dan mendengarkan kumpulan khotbah kapan saja dan di mana saja. Semua buku elektronik dan buku audio sepenuhnya gratis.

Anda dapat mendengarkan buku audio melalui pemutar di bawah ini. 🔻
Miliki buku cetak
Beli buku cetak di Amazon
Zamkati
 
Kalambulabwalo
1. Kodi Ampatuko ndi Otani Pamaso pa Mulungu? (1 Mafumu 11:1-13) 
2. Kodi Akristu Amene Akhulupilira Mwa Yesu Mkati mwa Chikonzero cha Nchito Yochokera Mkuganiza kwa Kuthupi Kwawo ndi Otani? (1 Mafumu 12:25-33) 
3. Kutsatira Zokhumba za Thupi Kuzakupangitsa kukhala Wampatuko Nthawi Imeneyo (1 Mafumu 12:1-18) 
4. Kodi ndi mu Uthenga Otani mu Umene Tsopano Mkukhulupilira? (1 Mafumu 13:33-34) 
5. Akristu a Masiku Ano Amene Anachosapo Mulungu N’kuikapo Zinthu Zopanda Pake ndi Opembeza Mafano Pamaso pa Mulungu (1 Mafumu 11:1-13) 
6. Kodi Mulungu Akupulumutsa Bwanji Ampatuko? (1 Mafumu 19:1-21) 
7. Muyenera Kukhulupilira Kuti Yohane M’batizi ndi Oimilirako Anthu Onse (Mateyu 11:1-19) 
8. Mitundu 7 ya Anthu Amene Adzatembeleledwa ndi Mulungu (Mateyu 23:1-36) 
9. Chilitsani Madzi Oipa ndi Mchere (2 Mafumu 2:19-22) 
 
Mu Baibulo, anthu a Isiraeli akunena kuti akupembeza Mulungu, koma pamapeto ake, anasatira Yerobowamu, anali kupembeza ana ang’ombe agolide. Mchoona, kopitila 2/3 ya mbiri ya Aisiraeli inali mbiri yakupembeza ana ang’ombe agolide, kuganiza kuti iwo ndi Mulungu. Pothera pake, ngakhalenso tsopanoli, akupitiliza kukhala ndi moyo kopanda kuzindikira choona kuti Yesu Khristu, amene anabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kuti ndi M’pulumutsi wawo oona. Kosasamala za ichi, kuli aYuda ambiri amene akuyembekezera za M’pulumutsi wawo, ngakhalenso tsopanoli. 
Kodi ndiyeno, chikhulupiliro chanu inu amene mkunena kuti mkutengako mbali mu Chikristu Mnthawiyi ya Chipangano cha Tsopano chii motani? Kodi tsopano mkukhulupilira mu ndi kusatira Mulungu mwakumvetsetsa koyenera kwa Iye? Ngati ai, kodi mwina mwake inu si mkupembeza ana ang’ombe agolide mwakusamvetsetsa iwo ngati Mulungu? Ngati muli choncho, ndiye kuti muyenera kudziwa za choona chakuti mkupembeza fano pamaso pa Mulungu ngati anthu a Isiraeli. Ndiye kuti, muyenera kubweleranso ndi kukumana ndi Ambuye amene anabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Ndikhulupilira kuti mdzakwanitsa kukhulupilira mu Choonadi ngati mwazindikiradi pamaso pa Mulungu cimene ndi Choonadi cha chipulumutso mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kodi si mdzatero? 
Ndifuna kuchitira umboni pamaso pa inu chikhulupiliro choona ndi Choonadi pa chapamutu, “Ampatuko, Amene anasatira machimo a Yerobowamu.” Mwanjira zonse, Ndikhulupilira mdzakhala anthu a chikhulupiliro chofanana ngati chija changa. 
Lebih

Buku-buku yang terkait dengan judul ini

The New Life Mission

Bagaimana Anda mengetahui tentang kami?

Bagaimana Anda mengetahui tentang kami?