Search

BUKU ELEKTRONIK DAN BUKU AUDIO GRATIS

Injil air dan Roh

Chichewa-Sango  1

[Chichewa-Sängö] KODI MWABADWADI MWATSOPANO MWA MADZI NDI MZIMU WOYERA? [Kusindikiza Kokonzedwanso Kwatsopano]-AKIRI ADU MO BIANI NA LEGE TI NGU NA YINGO AWE? [Fini lekengo]

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928226528 | Halaman 955

Unduh buku elektronik dan buku audio GRATIS

Pilih format file yang Anda inginkan dan unduh dengan aman ke perangkat seluler, PC, atau tablet Anda untuk membaca dan mendengarkan kumpulan khotbah kapan saja dan di mana saja. Semua buku elektronik dan buku audio sepenuhnya gratis.

Anda dapat mendengarkan buku audio melalui pemutar di bawah ini. 🔻
Miliki buku cetak
Beli buku cetak di Amazon
ZAM’KATIMU
 
Chigawo Choyamba — Maulaliki 
1. Choyamba Ife Tiyenera Kudziwa Machimo Athu kuti Tiomboledwe (Marko 7:8-9, 20-23)
2. Anthu Amabadwa Wochimwa (Marko 7:20-23)
3. Ngati Ife Tichita Zinthu Motsatira Lamulo, Kodi Ilo Lingatipulutse Ife? (Luka 10:25-30) 
4. Chiombolo cha Muyaya (Yohane 8:1-12) 
5. Ubatizo wa Yesu ndi Chitetezero cha Machimo (Mateyu 3:13-17)
6. Yesu Kristu Adadza mwa Madzi, Mwazi, ndi Mzimu Woyera (1 Yohane 5:1-12)
7. Ubatizo wa Yesu Ndi Chifaniziro cha Chipulumutso cha Ochimwa (1 Petro 3:20-22)
8. Uthenga Wabwino wa Chiombolo Chochuluka (Yohane 13:1-17)
 
Chigawo Chachiwiri — Mau Owonjezera
1. Kufotokoza Kowonjezera
2. Mafunso ndi Mayankho
 
(Chichewa)
Mutu waukulu wa bukuli ndi "kubadwa mwatsopano mwa Madzi ndi Mzimu Woyera." Ili ndi chiyambi chake pa mutuwu. Mwanjira ina, bukuli limatiwuza momveka bwino chomwe kubadwa mwatsopano kuli ndi mmene tingabadwire mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu Woyera molingana ndi Baibulo. Madzi amaimira ubatizo wa Yesu ku Yordano ndipo Baibulo limati machimo athu onse anaperekedwa kwa Yesu pamene Iye anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane anali woimira anthu onse ndiponso mdzukulu wa Aroni, Wansembe Wamkulu. Aroni anasanjika manja ake pamutu pa mbuzi yopereka nsembe ndipo anapititsira machimo onse a chaka cha Aisraeli pa iyo pa Tsiku la Chiyanjanitso. Ichi ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Ubatizo wa Yesu ndi chifaniziro cha kusanjika manja. Yesu anabatizidwa m`njira ya kusanjika manja ku Yordano. Choncho Iye anachotsa machimo onse a dziko lapansi kudzera mu ubatizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipire machimowo. Koma Akhristu ambiri sadziwa chifukwa chake Yesu anabatizidwa ndi Yohane Mbatizi mu Yordano. Ubatizo wa Yesu ndi mawu ofunika kwambiri a bukuli ndiponso gawo losatheka kuchotsa la Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu Woyera. Tikhoza kubadwa mwatsopano pokhapokha titakhulupirira mu ubatizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.
 
(Sango)
Kota mama tënë ti buku so ayeke « titene akiri adu zo na lege ti ngu na Yingo ». Aluti na ndö tënë so ayeke taa na gonda ni. Na mbeni ngobo ti tenengo ni, buku so atene na e avuru tarara nda ti ye so ayeke dungo zo ti fini ni  si nga tongana nyen si akiri adu zo na lege ti ngu na Yingo alingbi taa na Mbeti ti Nzapa. Ngu ayeke limo ti bateme ti Jezu na Jurden. Mbeti ti Nzapa atene atokua asiokpari ti e kue na li ti Jezu na ndembe so Jean-Batiste asara bateme na Jezu. Aaron azia maboko ti lo use kue na li ti koli-ngasa ti tokua si lo tokua asiokpari kue ti amara ti Israel ti ngu oko oko na li ti ngasa ni na lango ti mbongo asiokpari. So ayeke limo ti anzoni ye so ayeke ga. Bateme ti Jezu ayeke mara ti ziango maboko. Asara bateme na Jezu tongana ziango maboko na ngu ti Jurden. Nilaa, Lo mu asiokpari kue ti dunia na lege ti bateme ti lo na afâ lo na ndö keke ti kulusu ti futa ndali ti asiokpari ni. Me gbâ ti awamungo peko ti Kriste ahinga nga pepe ndani nyen si Jean-Batiste asara bateme na Jezu na ngu ti Jurden. Bateme ti Jezu ayeke kota tënë  ti ya ti buku so si nga ayeke mbage ti ye so ayeke na ngere ngangu na ya ti Nzoni Sango ti ngu na Yingo. E lingbi titene akiri adu e gi na mango na be na bateme ti Jezu nga na keke ti kulusu ti lo.
 
 Next 
Chichewa 2: BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
BWELERANI KU UTHENGA WABWINO WA MADZI NDI MZIMU
Lebih
Pemutar buku audio

Buku-buku yang terkait dengan judul ini

The New Life Mission

Bagaimana Anda mengetahui tentang kami?

Bagaimana Anda mengetahui tentang kami?