Search

مفت ای بُکس اور مفت آڈیو بُکس

یوحنا دا پہلا خط

چیچھیوا  14

Paul C. Jong’s Kukula Mumzimu Mundandanda wa 3 - Kalata Woyamba Wa Yohane (Ⅰ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239269 | ورقے 337

ڈاؤن لوڈ کرو مفت ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں

اپنی پسندیدہ فائل فارمیٹ چنو تے اپنے موبائل ڈیوائس، پی سی یا ٹیبلٹ تے محفوظ طریقے نال ڈاؤن لوڈ کرو تاں جو تسیں کدے وی، کتھے وی وعظاں دا مجموعہ پڑھ تے سن سکو۔ ساریاں ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں بلکل مفت نیں۔

🔻تسیں تھلے دتے گئے پلیئر راہیں آڈیو کتاب سن سکدے او۔
پرنٹڈ کتاب دے مالک بنو
ایمیزون تے پرنٹڈ کتاب خریدو
Zamakati
 
Kalambulabwalo

CHAPITALA 1
1. Yesu Khristu Ndi Mulungu (1 Yohane 1:1-10) 
2. Kodi Mulidi pa Mugwirizano ndi Mulungu? (1 Yohane 1:1-10) 
3. Mitundu Iwiri ya Kumvomereza (1 Yohane 1:8-10) 
4. Kuvomereza mu Choonadi (1 Yohane 1:8-10) 

CHAPITALA 2
1. Yesu Khristu Ndi Mulungu Woona (1 Yohane 2:1-5) 
2. Ambuye Athu Amene Anakhala Mthandizi Wathu (1 Yohane 2:1-17) 
3. Kodi Inu M’kukhala mu Lamulo La Mulungu? (1 John 2:7-11) 
4. Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za Mdziko (1 Yohane 2:15-17) 
5. Kodi Adani a Khristu Ndani (1 Yohane 2:18-29) 
 
Mtumwi Yohane ndi mumodzi wa atsogoleri aakulu mumzimu mu Chikhristu. Makalata onse atatu iye analemba akuchitilabe umboni wa wa Choonadi wa cha poyera ndi mumzimu ku woyera mu Mpingo wa Mulungu. Koma muli ndime zina zimene ndi zikosa kuti ife timasulire ndi kumvetsa.
Tingapereke 1Yohane 1:8 ngati chisanzo cha ndime zobvuta mu Makalata ya Yohane: Tikanena kuti: “Tilibe uchimo,” ndiye kuti tikudzinamiza ndipo mwa ife mulibe choonadi.” Ndimeyi ndiyobvuta kumvetsa, maka-maka ngati taigwiritsa nchito ku okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu.
Chisanzo chachiwiri ndi 1 Yohane 1:9, “Mulungu ndiwokhulupirika ndiponso wolungama, chotero tikavomereza machimo athu, adzatikhululukira ndi kutiyeretsa ku ntchito zonse zoipa.” Iyi yakhala ndime yakunenedwa pafupipafupi ngati ochimwa akufuna kupereka mfundo zabaibulo za mapemphero awo akulapa. Ndiyeno, ndimeyi ikutanthauza kuti ochimwa afunika kuvomereza machimo awo kuti akhululukidwe kumachimo awo amene anachita kodi? Kapena, kodi chikutanthauza kuti olungama amene okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu ayenera kuvomereza machimo awo? Tifunika kukhulupilira ndimeyi malinga ndi kamsulidwe ka Mzimu Woyera, Mlembi wa Baibulo, ndiponso kumalingaliro a Mtumwi Yohane.
Chisanzo cha chitatu cha ndime yobvuta ndi 1 Yohane 2:22, “Kodi wabodza angakhalenso ndani, kuposa amene amatsutsa kuti Yesu ndiye Khristu? Ameneyu ndiye wokana Khristu, amene amakana Atate ndi Mwana.” Ndimeyi ikulankhula za amene ndi adani a Mulungu. Ndimeyi ikufotokoza poyera kuti adani a Mulungu ndi onse aja sakhulupilira kuti Yesu ndi Mulungu. Ndipo ichi chikutanthauzanso kuti sakuthokoza Atate a Yesu Khristu ngati Mulungu.
Chachinayi ndi 1 Yohane 3:6 imene ikuti, “Yense wakukhala mwa Iye sachimwa yense wakuchimwa sanamuone Iye, ndipo sanamdziwe Iye.” Apa, ngati taona mawu, yense wakukhala mwa iye,” ndimeyi akuperekedwa ku olungama amene anayeretsedwa kumachimo awo onse mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Olungama sangakane chikhulupiliro chawo muzokhoma zilizonse cifukwa akukhulupilira mu uthenga woona. Kodi kungakhaledi ena amene sakuchita machimo ndi mathupi awo? Aliyense akuchita uchimo. Koma, okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu sangachite uchimo otero ngati wakukana uthenga woona.
ھور

اِس عنوان سے متعلقہ کتابیں

The New Life Mission

ساڈے سروے وچ حصہ پاؤ

تہانوں ساڈے بارے کنج پتہ چلیا؟