Search

مفت ای بُکس اور مفت آڈیو بُکس

پیدائش

چیچھیوا  22

Ziphunzitso pa Genesis (Ⅰ) - CHIFUNIRO Cha Utatu Oyera Ku Anthu

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239979 | ورقے 474

ڈاؤن لوڈ کرو مفت ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں

اپنی پسندیدہ فائل فارمیٹ چنو تے اپنے موبائل ڈیوائس، پی سی یا ٹیبلٹ تے محفوظ طریقے نال ڈاؤن لوڈ کرو تاں جو تسیں کدے وی، کتھے وی وعظاں دا مجموعہ پڑھ تے سن سکو۔ ساریاں ای-کتاباں تے آڈیو کتاباں بلکل مفت نیں۔

🔻تسیں تھلے دتے گئے پلیئر راہیں آڈیو کتاب سن سکدے او۔
پرنٹڈ کتاب دے مالک بنو
ایمیزون تے پرنٹڈ کتاب خریدو
Zamkati

Kalambulabwalo 

CHAPTER 1
1. Baibulo Ndilo Mawu a Chipulumutso, Osati Buku la Maphunziro a Zachilengedwe (Genesis 1:1-2) 
2. Kodi Munakhala Kuwala Mu Uthenga wa Choonadi? (Genesis 1:2-3) 
3. Kuchoka Ku Mphamvu ya Mdima kulowa Mu Ufumu wa Mwana (Genesis 1:2-5) 
4. Tsiku Loyamba: Pachiyambi Mulungu Analenga Kumwamba ndi Dziko Lapansi (Genesis 1:1-5) 
5. Madzi A Pamwamba pa Thambo ndi Madzi a Pansi pa Thambo (Genesis 1:6-8) 
6. Mulungu Analekanitsa Madzi Pa Tsiku Lachiwiri (Genesis 1:6-8) 
7. Kukwanilitsa Chifuniro cha Mulungu (Genesis 1:9-13) 
8. Kuti Tilowe M’kati Mwa Ntchito ya Mulungu (Genesis 1:9-13) 
9. Tingapulumutsidwe ku Uchimo Wathu Onse Pokhapo Ngati Tikudziwa Kuipa Kwathu Konse (Genesis 1:9-13) 
10. Kodi N’chiyani Chimene Atumiki a Mulungu Amene Akhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu Ayenera Kuchita (Genesis 1:14-19) 
11. Mulungu Akutipanga Kukhala Ziwiya Zaulemu (Genesis 1:16-19) 
12. Olungama Adzakhala Ndi Moyo Mwachikhulupiliro Chokha (Genesis 1:20-23) 
13. Ikani Mitima Yanu Pamaso pa Mulungu (Genesis 1:20-23) 
14. Miyoyo ya Anthu a Chikhulupiliro Amene Akhulupilira mu Mawu a Mulungu Ndi Mitima Yawo (Genesis 1:20-23) 
15. Chifukwa Chimene Mulungu Anatipangira Mofanana ndi Chifanizo Chake (Genesis 1:24-31) 
16. Tinapangidwa M’chifanizo cha Mulungu (Genesis 1:24-31) 
 
Mu Buku la Genesis, cholinga cimene Mulungu anatilengera chikupezeka. Ngati omanga manyumba apanga maonekedwe a nyumba kapena olemba ailemba, poyamba akukhala ndi nchito imene adzakwanilitsidwa mu maganizo awo sanayambedi kugwira nchito pa nchito yawoyo. Momwemo, Mulungu wathu nayenso anali nacho chipulumutso chathu mu maganizo Ache cha anthu ngakhalenso asanalenge kumwamba ndi dziko lapansi, ndipo Iye anapanga Adamu ndi Eve mwa cholingachi mu maganizo. Mulungu anali kufuna kumasulira kwa ife a malo a Kumwamba, amene sakuoneka ndi maso athu a thupi, mwakupanga chifanizo cha malo a padziko lapansi cimene tonse tingachione ndi kuchimvetsetsa.
Ngakhalenso dziko lisanakhalepo, Mulungu anali kufuna kupulumutsa anthu mwa ngwiro mwa kuwapatsa uthenga wa madzi ndi Mzimu ku mtima wa munthu aliyense. Chotero ngakhale kuti anthu onse anapangidwa kuchoka kufumbi, ayenera kuphunzira ndi kudziwa Choonadi cha uthenga wa madzi ndi Mzimu kuti aphindulire miyoyo yawo. Ngati anthu akupitiliza kukhala kopanda kudziwa ulamuliro wa Kumwamba, adzataya osati zinthu zokha zadziko lapansi, komanso zinthu zonse zimene zili Kumwamba.
ھور

اِس عنوان سے متعلقہ کتابیں

The New Life Mission

ساڈے سروے وچ حصہ پاؤ

تہانوں ساڈے بارے کنج پتہ چلیا؟