Search

無料の電子書籍とオーディオブック

使徒パウロのローマ人への手紙

チェワ語  6

Chilungamo cha Mulungu Chomwe Chaonetsedwa mu Aroma - Ambuye Wathu Yemwe Wakhala Chilungamo cha Mulungu (Ⅱ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 8983143215 | ページ 377

電子書籍とオーディオブックを無料でダウンロード

お好みのファイル形式を選択し、モバイル端末、PC、タブレットに安全にダウンロードして、説教集をいつでもどこでも読んだり聴いたりすることができます。すべての電子書籍とオーディオブックは完全無料です。

下記のプレーヤーでオーディオブックを聴くことができます。🔻
ペーパーバックを所有
Zamkatimu
 
Mau Oyamba 

Mutu 7
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 7 
2. Mfundo ya Chikhulupiliro cha Paulo: Kulumikizana ndi Kristu titafa ku uchimo (Aroma 7:1-4) 
3. Chifukwa Chomwe Tingatamandire Ambuye (Aroma 7:5-13) 
4. Thupi lathu Lomwe Limatumikira Thupi Lokha Basi (Aroma 7:14-25) 
5. Thupi Limatumikira Lamulo la Uchimo (Aroma 7:24-25) 
6. Tamandani Ambuye, Mpulumutsi wa Ochimwa (Aroma 7:14-8:2) 

Mutu 8
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 8 
2. Chilungamo cha Mulungu, Chikwaniritso cha Chofunikira Cholungama cha Lamulo (Aroma 8:1-4) 
3. Kodi m’Kristu Ndindani? (Aroma 8:9-11) 
4. Chisamaliro cha Thupi chiri Imfa, koma Chisamaliro cha Mzimu chiri Moyo ndi Mtendere (Aroma 8:4-11) 
5. Kuyenda mu Chilungamo cha Mulungu (Aroma 8:12-16) 
6. Iwo amene amalowa Ufumu wa Mulungu (Aroma 8:16-27) 
7. Kubwera Kwachiwiri kwa Ambuye komanso Ufumu wa Zakachikwi (Aroma 8:18-25) 
8. Mzimu Woyera Umene Umathandiza Olungama (Aroma 8:26-28) 
9. Zinthu Zonse Zithandizana Kuwachitira Ubwino (Aroma 8:28-30) 
10. Ziphunzitso Zolakwika (Aroma 8:29-30) 
11. Chikondi Chosatha (Aroma 8:31-34) 
12. Ndindani Angayese Kutsutsana Nafe? (Aroma 8:31-34) 
13. Ndindani Amene Adzasiyanitsa Olungama ku Chikondi cha Kristu? (Aroma 8:35-39) 

Mutu 9
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 9 
2. Tiyenera Kudziwa Kuti Kukonzedweratu Kunakonzedwa Mkati mwa Chilungamo cha Mulungu (Aroma 9:9-33) 
3. Kodi ndi kulakwitsa Mulungu Kukonda Yakobo? (Aroma 9:30-33) 

Mutu 10
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 10 
2. Chikhulupiliro Chenicheni Chidza ndi Mbiri (Aroma 10:16-21) 

Mutu 11
1. Kodi Israyeli Adzapulumutsidwa? 

Mutu 12
1. Konzani Mtima Wanu Pamaso pa Mulungu 

Mutu 13
1. Khalani Chifukwa cha Chilungamo cha Mulungu 

Mutu 14
1. Musaweruzane Wina ndi Mnzake 

Mutu 15
1. Tiyeni Tifalitse Uthenga Wabwino ku Dziko Lonse Lapansi 

Mutu 16
1. Mulankhulane Wina ndi Mnzake 
 
Chilungamo Cha Mulungu chimaonekera ndipo chisiyana ndichija cha munthu. Chilungamo cha Mulungu chavumbulidwa muuthenga wamadzi ndi Mzimu, umene unakwaniritsidwa ndi kubadizidwa kwa Yesu kuli Yohane ndi mwazi Wake Pamtanda. Tibwerere kuchikhulupiliro cha Chilungamo cha Mulungu, tisachedwe.
Kodi ukudziwa ninji Yesu anabadizidwa ndi Yohne Mbadizi? Ngati Yohane sanabadize Yesu, machismo athu akanapatsidwa kwaiye. Yohane Mbadizi ndiye munthu wamkulu kupambana onse, ndipo ubadizo anapatsa Yesu unalingana ndichifuniro cha Mulungu kuti machismo athu apatsidwe kwa Yesu.
Yesu anabadizidwa kuti asenze machismo a anthu onse papewa pake, ndikufa pamtanda kulipa machismo. Zinthu zonsezi zasintha maganizo anga akuti kubadwanso nciani, chifukwa ndinangodziwa za mwazi pa Mtanda. Tsopano Mulungu wakupunzitsani kuti Chilungamo chake nhiani kuti tidziwe ndikukhulupilira mu Chilungamo chakecho mwatunthu. Ndithokoza Ambuye chifukwa chamadalitso onsewa.
もっと見る
オーディオブックプレーヤー

このタイトルに関連する書籍

The New Life Mission

アンケートに答える

当サイトをどのようにお知りになりましたか?