Search

無料の電子書籍とオーディオブック

マタイによる福音書

チェワ語  29

ULALIKI PA UTHENGA WABWINO WA MATEYU (III) - NDIWOTANI UTHENGA WABWINO OMWE UMAPANGITSA AKRISTU KUKHALA ANGWIRO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928241040 | ページ 386

電子書籍とオーディオブックを無料でダウンロード

お好みのファイル形式を選択し、モバイル端末、PC、タブレットに安全にダウンロードして、説教集をいつでもどこでも読んだり聴いたりすることができます。すべての電子書籍とオーディオブックは完全無料です。

下記のプレーヤーでオーディオブックを聴くことができます。🔻
ペーパーバックを所有
Amazonでペーパーバックを購入
Zamkatimu
 
Mau oyamba 

CHAPITALA 14
1. Milomo Ya Ansembe Auzimu Iyenera Kusunga Chidziwitso Cha Choonadi (Mateyu 14:1-12) 
2. Ndi Chifukwa Chiani Yesu Anachita Chozizwa Cha Mikate Isanu Ndi Nsomba Ziwiri? (Mateyu 14:13-33) 
 
CHAPITALA 15
1. Mulungu Watipatsa Ife Madalitso Opanda Malire (Mateyu 15:32-39) 

CHAPITALA 16
1. Tiyenera Kusamalira Ntchito Ya Mulungu Choyamba (Mateyu 16:21-25) 
2. Chikhulupiliro Chodzikana-Tokha (Mateyu 16:21-27) 
3. Chikondi Cha Petro Kwa Yesu (Mateyu 16:21-27) 
4. Ngati Munthu Afuna Kutsata Ine, Adzikane Yekha! (Mateyu 16:21-28) 
5. Dzikaneni Nokha Ndi Kutsata Ambuye (Mateyu 16:24-27) 
6. Chikhulupiliro Chokha Basi Chimapulumutsa Ife ku Uchimo (Mateyu 16:24-27) 

CHAPITALA 17
1. M’mene Tingalandirire Mzimu Woyera (Mateyu 17:1-13) 
2. Yohane Mbatizi, Amene Anadza M’njira Ya Chilungamo (Mateyu 17:1-13) 

CHAPITALA 18
1. Iwo Amene Chikhulupiliro Chao Chiri Monga Cha Kamwana (Mateyu 18:1-4) 

CHAPITALA 19
1. Iwo Amene Ali Achuma Mu Ntchito Zao Zabwino za Thupi Sangalowe Kumwamba (Mateyu 19:16-30) 

CHAPITALA 20
1. Khalani Chifukwa Cha Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Mateyu 20:20-28) 
 
Mtumwi Mateyu akutiuza ife kuti Mau a Yesu analankhulidwa kwa aliyense m’dziko lino, popeza Iye ankaona Yesu monga Mfumu ya mafumu. Tsopano, Akristu dziko lonse lapansi, amene angobadwa mwatsopano pokhulupilira mu uthenga wabwino wa madzi ndi Mzimu omwe tikufalitsa, indedi akufunitsitsa kudya mkate wamoyo. Koma ndikobvuta kwa iwo kukhala ndi chiyanjano ndi ife mu uthenga wabwino weni weni, popeza iwo onse ali kutali ndi ife. Choncho, kuti tikumane ndi zofunika zauzimu za anthu amenewa a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu,  ulaliki m’buku limeneli wakonzedwa monga mkate watsopano wa moyo kwa iwo kuti usamalire kukula kwao kwauzimu. Mlembi amanena kuti iwo amene alandira chikhululukiro cha machimo ao pokhulupilira m’Mau a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ayenera kudya Mau Ake angwiro pofuna kuteteza chikhulupiliro chao komanso kuchita bwino m’miyoyo yao yauzimu. Buku limeneli lidzapereka mkate weni weni wamoyo wauzimu kwa inu nonse amene mwakhala anthu olemekezeka a Mfumu mwa chikhulupiliro. Kudzera mu Mpingo Wake ndi akapolo Ake, Mulungu adzapitiriza kupereka kwa inu mkate umenewu wamoyo. Lolani madalitso a Mulungu akhale pa inu nonse amene mwabadwa mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu, amene mukufuna kukhala ndi chiayanjano chauzimu ndi ife mwa Yesu Kristu.
もっと見る
オーディオブックプレーヤー

このタイトルに関連する書籍

The New Life Mission

アンケートに答える

当サイトをどのようにお知りになりましたか?