Search

БЕЗКОШТОВНІ ЕЛЕКТРОННІ КНИГИ ТА АУДІОКНИГИ

Лист апостола Павла до римлян

Чичева  6

Chilungamo cha Mulungu Chomwe Chaonetsedwa mu Aroma - Ambuye Wathu Yemwe Wakhala Chilungamo cha Mulungu (Ⅱ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 8983143215 | Сторінки 377

Завантажте електронні книги та аудіокниги БЕЗКОШТОВНО

Виберіть бажаний формат файлу та безпечно завантажте на мобільний пристрій, ПК або планшет, щоб читати та слухати колекції проповідей будь-де та будь-коли. Всі електронні книги та аудіокниги повністю безкоштовні.

Ви можете прослухати аудіокнигу через плеєр нижче. 🔻
Майте друковану книгу
Zamkatimu
 
Mau Oyamba 

Mutu 7
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 7 
2. Mfundo ya Chikhulupiliro cha Paulo: Kulumikizana ndi Kristu titafa ku uchimo (Aroma 7:1-4) 
3. Chifukwa Chomwe Tingatamandire Ambuye (Aroma 7:5-13) 
4. Thupi lathu Lomwe Limatumikira Thupi Lokha Basi (Aroma 7:14-25) 
5. Thupi Limatumikira Lamulo la Uchimo (Aroma 7:24-25) 
6. Tamandani Ambuye, Mpulumutsi wa Ochimwa (Aroma 7:14-8:2) 

Mutu 8
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 8 
2. Chilungamo cha Mulungu, Chikwaniritso cha Chofunikira Cholungama cha Lamulo (Aroma 8:1-4) 
3. Kodi m’Kristu Ndindani? (Aroma 8:9-11) 
4. Chisamaliro cha Thupi chiri Imfa, koma Chisamaliro cha Mzimu chiri Moyo ndi Mtendere (Aroma 8:4-11) 
5. Kuyenda mu Chilungamo cha Mulungu (Aroma 8:12-16) 
6. Iwo amene amalowa Ufumu wa Mulungu (Aroma 8:16-27) 
7. Kubwera Kwachiwiri kwa Ambuye komanso Ufumu wa Zakachikwi (Aroma 8:18-25) 
8. Mzimu Woyera Umene Umathandiza Olungama (Aroma 8:26-28) 
9. Zinthu Zonse Zithandizana Kuwachitira Ubwino (Aroma 8:28-30) 
10. Ziphunzitso Zolakwika (Aroma 8:29-30) 
11. Chikondi Chosatha (Aroma 8:31-34) 
12. Ndindani Angayese Kutsutsana Nafe? (Aroma 8:31-34) 
13. Ndindani Amene Adzasiyanitsa Olungama ku Chikondi cha Kristu? (Aroma 8:35-39) 

Mutu 9
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 9 
2. Tiyenera Kudziwa Kuti Kukonzedweratu Kunakonzedwa Mkati mwa Chilungamo cha Mulungu (Aroma 9:9-33) 
3. Kodi ndi kulakwitsa Mulungu Kukonda Yakobo? (Aroma 9:30-33) 

Mutu 10
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 10 
2. Chikhulupiliro Chenicheni Chidza ndi Mbiri (Aroma 10:16-21) 

Mutu 11
1. Kodi Israyeli Adzapulumutsidwa? 

Mutu 12
1. Konzani Mtima Wanu Pamaso pa Mulungu 

Mutu 13
1. Khalani Chifukwa cha Chilungamo cha Mulungu 

Mutu 14
1. Musaweruzane Wina ndi Mnzake 

Mutu 15
1. Tiyeni Tifalitse Uthenga Wabwino ku Dziko Lonse Lapansi 

Mutu 16
1. Mulankhulane Wina ndi Mnzake 
 
Chilungamo Cha Mulungu chimaonekera ndipo chisiyana ndichija cha munthu. Chilungamo cha Mulungu chavumbulidwa muuthenga wamadzi ndi Mzimu, umene unakwaniritsidwa ndi kubadizidwa kwa Yesu kuli Yohane ndi mwazi Wake Pamtanda. Tibwerere kuchikhulupiliro cha Chilungamo cha Mulungu, tisachedwe.
Kodi ukudziwa ninji Yesu anabadizidwa ndi Yohne Mbadizi? Ngati Yohane sanabadize Yesu, machismo athu akanapatsidwa kwaiye. Yohane Mbadizi ndiye munthu wamkulu kupambana onse, ndipo ubadizo anapatsa Yesu unalingana ndichifuniro cha Mulungu kuti machismo athu apatsidwe kwa Yesu.
Yesu anabadizidwa kuti asenze machismo a anthu onse papewa pake, ndikufa pamtanda kulipa machismo. Zinthu zonsezi zasintha maganizo anga akuti kubadwanso nciani, chifukwa ndinangodziwa za mwazi pa Mtanda. Tsopano Mulungu wakupunzitsani kuti Chilungamo chake nhiani kuti tidziwe ndikukhulupilira mu Chilungamo chakecho mwatunthu. Ndithokoza Ambuye chifukwa chamadalitso onsewa.
Більше
Безкоштовна друкована книга
Додати цю друк. книгу в кошик

Книги, схожі на цю

The New Life Mission

зьміть участь у нашому опитуванні

Як ви дізналися про нас?