Search

مفتایبُکساورمفتآڈیوبُکس

متّی کی انجیل

چیچھیوا  29

ULALIKI PA UTHENGA WABWINO WA MATEYU (III) - NDIWOTANI UTHENGA WABWINO OMWE UMAPANGITSA AKRISTU KUKHALA ANGWIRO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928241040 | صفحات 386

ڈاؤن لوڈ کریں مفت ای بکس اور آڈیو بکس

اپنی پسندیدہ فائل فارمیٹ منتخب کریں اور اپنے موبائل ڈیوائس، پی سی یا ٹیبلٹ پر محفوظ طریقے سے ڈاؤن لوڈ کریں تاکہ آپ کہیں بھی، کبھی بھی خطبات کا مجموعہ پڑھ اور سن سکیں۔ تمام ای بکس اور آڈیو بکس بالکل مفت ہیں۔

🔻آپ نیچے دیئے گئے پلیئر کے ذریعے آڈیو بک سن سکتے ہیں۔
پرنٹڈ کتاب کے مالک بنیں
ایمیزون پر پرنٹڈ کتاب خریدیں
Zamkatimu
 
Mau oyamba 

CHAPITALA 14
1. Milomo Ya Ansembe Auzimu Iyenera Kusunga Chidziwitso Cha Choonadi (Mateyu 14:1-12) 
2. Ndi Chifukwa Chiani Yesu Anachita Chozizwa Cha Mikate Isanu Ndi Nsomba Ziwiri? (Mateyu 14:13-33) 
 
CHAPITALA 15
1. Mulungu Watipatsa Ife Madalitso Opanda Malire (Mateyu 15:32-39) 

CHAPITALA 16
1. Tiyenera Kusamalira Ntchito Ya Mulungu Choyamba (Mateyu 16:21-25) 
2. Chikhulupiliro Chodzikana-Tokha (Mateyu 16:21-27) 
3. Chikondi Cha Petro Kwa Yesu (Mateyu 16:21-27) 
4. Ngati Munthu Afuna Kutsata Ine, Adzikane Yekha! (Mateyu 16:21-28) 
5. Dzikaneni Nokha Ndi Kutsata Ambuye (Mateyu 16:24-27) 
6. Chikhulupiliro Chokha Basi Chimapulumutsa Ife ku Uchimo (Mateyu 16:24-27) 

CHAPITALA 17
1. M’mene Tingalandirire Mzimu Woyera (Mateyu 17:1-13) 
2. Yohane Mbatizi, Amene Anadza M’njira Ya Chilungamo (Mateyu 17:1-13) 

CHAPITALA 18
1. Iwo Amene Chikhulupiliro Chao Chiri Monga Cha Kamwana (Mateyu 18:1-4) 

CHAPITALA 19
1. Iwo Amene Ali Achuma Mu Ntchito Zao Zabwino za Thupi Sangalowe Kumwamba (Mateyu 19:16-30) 

CHAPITALA 20
1. Khalani Chifukwa Cha Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Mateyu 20:20-28) 
 
Mtumwi Mateyu akutiuza ife kuti Mau a Yesu analankhulidwa kwa aliyense m’dziko lino, popeza Iye ankaona Yesu monga Mfumu ya mafumu. Tsopano, Akristu dziko lonse lapansi, amene angobadwa mwatsopano pokhulupilira mu uthenga wabwino wa madzi ndi Mzimu omwe tikufalitsa, indedi akufunitsitsa kudya mkate wamoyo. Koma ndikobvuta kwa iwo kukhala ndi chiyanjano ndi ife mu uthenga wabwino weni weni, popeza iwo onse ali kutali ndi ife. Choncho, kuti tikumane ndi zofunika zauzimu za anthu amenewa a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu,  ulaliki m’buku limeneli wakonzedwa monga mkate watsopano wa moyo kwa iwo kuti usamalire kukula kwao kwauzimu. Mlembi amanena kuti iwo amene alandira chikhululukiro cha machimo ao pokhulupilira m’Mau a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ayenera kudya Mau Ake angwiro pofuna kuteteza chikhulupiliro chao komanso kuchita bwino m’miyoyo yao yauzimu. Buku limeneli lidzapereka mkate weni weni wamoyo wauzimu kwa inu nonse amene mwakhala anthu olemekezeka a Mfumu mwa chikhulupiliro. Kudzera mu Mpingo Wake ndi akapolo Ake, Mulungu adzapitiriza kupereka kwa inu mkate umenewu wamoyo. Lolani madalitso a Mulungu akhale pa inu nonse amene mwabadwa mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu, amene mukufuna kukhala ndi chiayanjano chauzimu ndi ife mwa Yesu Kristu.
مزید

ایس سرناویں نال رلدیاں ملدیاں کتاباں

The New Life Mission

ہمارے سروے میں حصہ ڈالیں

آپ کو ہمارے بارے میں کیسے معلوم ہوا؟