• 所有新生命宣教会 The New Life Mission 网站上的电子书和有声书均可免费下载
  • 探索以多种语言提供的全球性讲道
  • 查看我们已翻译成27种语言的网站
  • 第1卷新修订版已全新推出
Search

免费电子书和有声读物

创世记

奇切瓦语  22

Ziphunzitso pa Genesis (Ⅰ) - CHIFUNIRO Cha Utatu Oyera Ku Anthu

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239979 | 页码 474

下载免费电子书和有声读物

选择您喜欢的文件格式,安全下载到手机、电脑或平板电脑,随时随地阅读和收听讲道集。所有电子书和有声读物都完全免费。

您可以通过下方播放器收听有声读物。🔻
拥有平装书
在亚马逊购买平装书
Zamkati

Kalambulabwalo 

CHAPTER 1
1. Baibulo Ndilo Mawu a Chipulumutso, Osati Buku la Maphunziro a Zachilengedwe (Genesis 1:1-2) 
2. Kodi Munakhala Kuwala Mu Uthenga wa Choonadi? (Genesis 1:2-3) 
3. Kuchoka Ku Mphamvu ya Mdima kulowa Mu Ufumu wa Mwana (Genesis 1:2-5) 
4. Tsiku Loyamba: Pachiyambi Mulungu Analenga Kumwamba ndi Dziko Lapansi (Genesis 1:1-5) 
5. Madzi A Pamwamba pa Thambo ndi Madzi a Pansi pa Thambo (Genesis 1:6-8) 
6. Mulungu Analekanitsa Madzi Pa Tsiku Lachiwiri (Genesis 1:6-8) 
7. Kukwanilitsa Chifuniro cha Mulungu (Genesis 1:9-13) 
8. Kuti Tilowe M’kati Mwa Ntchito ya Mulungu (Genesis 1:9-13) 
9. Tingapulumutsidwe ku Uchimo Wathu Onse Pokhapo Ngati Tikudziwa Kuipa Kwathu Konse (Genesis 1:9-13) 
10. Kodi N’chiyani Chimene Atumiki a Mulungu Amene Akhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu Ayenera Kuchita (Genesis 1:14-19) 
11. Mulungu Akutipanga Kukhala Ziwiya Zaulemu (Genesis 1:16-19) 
12. Olungama Adzakhala Ndi Moyo Mwachikhulupiliro Chokha (Genesis 1:20-23) 
13. Ikani Mitima Yanu Pamaso pa Mulungu (Genesis 1:20-23) 
14. Miyoyo ya Anthu a Chikhulupiliro Amene Akhulupilira mu Mawu a Mulungu Ndi Mitima Yawo (Genesis 1:20-23) 
15. Chifukwa Chimene Mulungu Anatipangira Mofanana ndi Chifanizo Chake (Genesis 1:24-31) 
16. Tinapangidwa M’chifanizo cha Mulungu (Genesis 1:24-31) 
 
Mu Buku la Genesis, cholinga cimene Mulungu anatilengera chikupezeka. Ngati omanga manyumba apanga maonekedwe a nyumba kapena olemba ailemba, poyamba akukhala ndi nchito imene adzakwanilitsidwa mu maganizo awo sanayambedi kugwira nchito pa nchito yawoyo. Momwemo, Mulungu wathu nayenso anali nacho chipulumutso chathu mu maganizo Ache cha anthu ngakhalenso asanalenge kumwamba ndi dziko lapansi, ndipo Iye anapanga Adamu ndi Eve mwa cholingachi mu maganizo. Mulungu anali kufuna kumasulira kwa ife a malo a Kumwamba, amene sakuoneka ndi maso athu a thupi, mwakupanga chifanizo cha malo a padziko lapansi cimene tonse tingachione ndi kuchimvetsetsa.
Ngakhalenso dziko lisanakhalepo, Mulungu anali kufuna kupulumutsa anthu mwa ngwiro mwa kuwapatsa uthenga wa madzi ndi Mzimu ku mtima wa munthu aliyense. Chotero ngakhale kuti anthu onse anapangidwa kuchoka kufumbi, ayenera kuphunzira ndi kudziwa Choonadi cha uthenga wa madzi ndi Mzimu kuti aphindulire miyoyo yawo. Ngati anthu akupitiliza kukhala kopanda kudziwa ulamuliro wa Kumwamba, adzataya osati zinthu zokha zadziko lapansi, komanso zinthu zonse zimene zili Kumwamba.
更多

与该标题相关的书籍

The New Life Mission

参加我们的调查

您是如何了解到我们的?