Search

KOSTENLOSE E-BOOKS UND HÖRBÜCHER

Der Brief von Paulus dem Apostel an die Epheser

Chichewa  28

Chimene Mulungu Mtatu Anatichitira Ife - Ziphunzitso pa Aefeso (II)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240234 | Seiten 442

Laden Sie E-Books und Hörbücher KOSTENLOS herunter

Wählen Sie Ihr bevorzugtes Dateiformat und laden Sie es sicher auf Ihr Mobilgerät, PC oder Tablet herunter, um die Predigtsammlungen jederzeit und überall zu lesen und zu hören. Alle E-Books und Hörbücher sind völlig kostenlos.

Sie können das Hörbuch über den Player unten anhören. 🔻
Besitzen Sie ein Taschenbuch
Kaufen Sie ein Taschenbuch auf Amazon
Zamkati
 
Mawu Oyamba
1. Chipulumutso Chathu Chinakonzedwa Mu Chilungamo cha Yesu Ngakhalenso Pamene Dziko Lisanakhazikitsidwe (Aefeso 1:1-4) 
2. Takhala Akatundu a Mulungu mwa Chisomo Chake (Aefeso 1:1-14) 
3. Tinapulumutsidwa Kupitira mu Chikondi ndi Nsembe ya Mulungu (Aefeso 1:1-6) 
4. Tithokoza Mulungu Pakutiitana Ngati Mamembala a M’pingo Wake (Aefeso 1:20-23) 
5. Tili Ndichiombolo Mogwirizana Ndi Chuma cha Chisomo cha Mulungu (Aefeso 1:7-14) 
6. Kodi tinapangidwira Nchito Yolungama ya Ambuye? (Aefeso 2:1-10) 
7. Tiyenera Kudziwa Mphamvu ndi Chisomo cha Mulungu mu Umoyo Wathu Wachikhulupiliro (Aefeso 2:1-22) 
8. Kodi Tinali Mtundu wa Anthu Otani Pamaso pa Mulungu? (Aefeso 2:1-7) 
9. Takhala Osadziwika Kwa Mulungu Atate Cifukwa cha Machimo Athu (Aefeso 2:14-22) 
10. Madalitso Osaneneka a Khristu Ali M’mtima wa Oyera Aliyense Amene Akukhulupilira mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Aefeso 3:1-21) 
11. Tetezani Chikhulupiliro Chanu mu Umoyo Wanu (Aefeso 4:1-6) 
12. Tsanzirani Mulungu Ngati Ana Ake Okondedwa (Aefeso 5:1-2) 
13. Musatengeko Mbali Kumachimo Adziko (Aefeso 5:1-14) 
14. Kodi Kukhala mwa Kudzaza ndi Mzimu Chitanthauza Chiyani Kwenikweni? (Aefeso 5:1-21) 
15. Iwo Amene Akukhala mwa Kudzaza ndi Mzimu (Afeso 5:15-21) 
16. Tsutsanani ndi Machenjera a Satana (Aefeso 6:10-17) 
 
Kodi Mkudziwa M’mene Ulili M’pingo wa Mulungu?
 
Mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, muyenera kukhala ndi maso anu akuuzimu masiku onse otseguka. Ngati munalandira chikhululukiro cha machimo anu mwa kukhulupilira moona mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, ndiye kuti mdzatha kuzindikira M'pingo wa Mulungu moyenera; apo bii, simukanatha kudziwa moyenera imene ndi mipingo yaboza.
Masiku ano, Mulungu anakhazikitsa M'pingo Wake pachikhulupiliro cha okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. M'pingo wa Mulungu ndi kusonkhana kwa aja amene anapulumutsidwa mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Chotero, ngati mitima yanu tsopano ili ndi chikhulupiliro mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, ndiye kuti kenako mungakhale ndi chikhulupiliro mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kenako mungakhale moyo woona wachikhulupiliro. Moyo otero wachikhulupiliro ndi wotheka mu M'pingo wa Mulungu mokha. Moonjezera, chikhulupiliro chotere chokha chikutiyeneretsa kukakhala kwa muyaya mu Ufumu wa Ambuye. Kupitira muchikhulupiliro ichi, tiyenera kulandira chikondi cha chipulumutso ndi madalitso onse auzimu a Kumwamba kuchokera kwa Mulungu Atate, kwa Yesu Khristu, ndi ku Mzimu Woyera. 
Mehr

Bücher zu diesem Titel

The New Life Mission

Nehmen Sie an unserer Umfrage teil

Wie haben Sie von uns erfahren?