Search

VITABU PEPE NA VITABU VYA SAUTI BURE

Waraka wa Paulo Mtume kwa Wagalatia

Chichewa  16

Ziphunzitso mu Agalatiya - Kuchoka Kumdulidwe wa Kuthupi Kufika Kuchiphunzitso Cha Kulapa (Ⅰ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239474 | Kurasa 463

Pakua vitabu pepe na vitabu vya sauti BURE

Chagua muundo wa faili unaopendelea na upakue salama kwenye simu yako, kompyuta au kompyuta kibao kusoma na kusikiliza mkusanyiko wa mahubiri wakati wowote na mahali popote. Vitabu vyote pepe na vitabu vya sauti ni bure kabisa.

Unaweza kusikiliza kitabu cha sauti kupitia kichezaji hapa chini. 🔻
Miliki kitabu kilichochapishwa
Nunua kitabu kilichochapishwa kwenye Amazon
Zamkati
 
Kalambulabwalo 

CHAPITALA 1
1. Ambuye Anatilanditsa Kudzikoli Loipa (Galatiya 1:1-5) 
2. Kodi Chikhulupiliro Chanu Sichili Chofanana ndi Cha Amudulidwe Mwina? (Galatiya 1:1-5) 
3. Ambuye Anatilanditsa Mwa Ungwiro ndiponso Mwa Kamodzi Kokha (Galatiya 1:3-5) 
4. Sipangakhalenso Uthenga Wina Koma Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 1:6-10) 
5. Aja Amene Mitima Yawo Inaikidwa Ngati Atumiki a Mulungu (Galatiya 1:10-12) 
6. Chikhulupiliro Cha Mtumwi Paulo Ndi Chenjezo Lake ku Amudulidwe (Galatiya 1:1-17) 
7. Moyo Wachikhulupiriro Chachilamulo Ubweretsa Matemberero Okha (Galatiya 1:1-24) 

CHAPITALA 2
1. Chifukwa N’chiyani Mtumwi Paulo Anasura a Zachilamulo? (Galatiya 2:1-10) 
2. Tanthauzo Leni-leni la Chikhulupiliro cha Paulo (Galatiya 2:20) 
3. Mwachikhulupiliro mu Mwana wa Mulungu, Kodi Tinafa ndi Kuukitsidwa Limodzi Ndi Iye? (Galatiya 2:20) 
4. Munthu Samayetsedwa Olungama ndi Nchito za Chilamulo Koma mwa Chikhulupiliro mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 2:11-21) 
5. Tikuyetsedwa Wolungama mwa Chikhulupiliro Choyera Chokha (Galatiya 2:11-21) 

CHAPITALA 3
1. Masiku Onse Khalani Moyo wanu Mwa Chikhulupiliro mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 3:1-11) 
2. Kodi Kupanda Kanthu kwa Mitima Yathu Kukuzimiririka Nthawi Yotani? (Galatiya 3:23-29) 
3. Tsopano Sitiyenera Kukhalanso Pansi pa Matembelelo a Chilamulo (Galatiya 3:1-29) 
 
Chiphunzitso cha Kulapa Ndichokwanira Kukupanhitsani kuti Mtore Matenda a Kuuzimu.

Anthu mdziko lonse ali ndi mantha ndi tudoyo ngati SARS, cifukwa angafe mwamusanga mwa kuonetsedwa ku tudoyo totero tosaoneka.
Chimodzimodzi, Akristu masiku ano kudzungulira dziko lonse akufa mu mathupi awo ndiponso mu mzimu mwa kudwara ndi chiphunzitso cha kulapa. Kodi munali kudziwa kuti chiphunzitso cha kulapa ndi cholakwika moteromu?
Kodi mkudziwa amene anapangitsa Akristu kugwera mu dzenje lolowelera la chisokonezo cha mu mzimu. Ndi Akristu ochimwa iwo okha amene akupemphera mapemphero akulapa tsiku ndi tsiku kuti ayeretsedwe kumachimo awo a payekha payekha pamene akunena kuti okhulupilira mwa Yesu Khristu ngati M’pulumutsi wawo.
Chotero, muyenera kulandira chikhululukiro cha machimo mwa kukhulupilira mu Mawu a uthenga wa madzi ndi Mzimu umene Mulungu anatipatsa pachiyambi. Si muyenera kutaya mpata odalitsidwa okhala obadwa mwatsopano. Tonsefe tiyenera kumasulidwa kuchisokonezo cha mu mzimu mwa kukhulupilira mu Choonadi cha uthenga wa madzi ndi Mzimu. Tiyenera kuyangana pa kuwala konyezimira kwa Choonadi, cimene chinabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, titathawako kunjira ya chisokonezo cha mu mzimu.
Zaidi

Vitabu vinavyohusiana na kichwa hiki

The New Life Mission

Shiriki katika utafiti wetu

Ulitujuaje?