Search

ΔΩΡΕΑΝ ΗΛΕΚΤΡΟΝΙΚΑ ΒΙΒΛΙΑ ΚΑΙ ΗΧΗΤΙΚΑ ΒΙΒΛΙΑ

Η Αποκάλυψη

Τσιτσέουα  7

Ndemanga ndi Ulaliki pa Buku la Chibvumbulutso - KODI NYENGO YA WOTSUTSAKRISTU, KUFERA CHIKHULUPILIRO, MKWATULO KOMANSO UFUMU WA ZAKACHIKWI IKUDZA? ( I )

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928231294 | Σελίδες 369

Κατεβάστε ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία ΔΩΡΕΑΝ

Επιλέξτε την προτιμώμενη μορφή αρχείου και κατεβάστε με ασφάλεια στην κινητή συσκευή, τον υπολογιστή ή το tablet σας για να διαβάσετε και να ακούσετε τις συλλογές κηρυγμάτων οποιαδήποτε στιγμή και οπουδήποτε. Όλα τα ηλεκτρονικά βιβλία και ηχητικά βιβλία είναι εντελώς δωρεάν.

Μπορείτε να ακούσετε το ηχητικό βιβλίο μέσω του προγράμματος αναπαραγωγής παρακάτω. 🔻
Αποκτήστε ένα χαρτόδετο βιβλίο
Αγοράστε ένα χαρτόδετο βιβλίο στο Amazon
Zamkatimu 
 
Mau Oyamba 

MUTU 1
1. Imvani Mau a Chibvumbulutso cha Mulungu (Civumbulutso 1:1-20) 
2. Tiyenera Kudziwa Nyengo Zisanu Ndi Ziwiri 

MUTU 2
1. Kalata ya Mpingo wa ku Efeso (Chivumbulutso 2:1-7) 
2. Chikhulupiliro Chomwe Chingalandire Kuphedwa Chifukwa cha Kristu 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Smurna (Chibvumbuutso 2:8-11) 
4. Khalani Okhulupirika kufikira Imfa 
5. Ndindani Wopulumutsidwa ku Uchimo? 
6. Kalata ya Mpingo wa ku Pergamo (Chibvumbulutso 2:12-17) 
7. Osatira Chiphunzitso cha Anikolai 
8. Kalata ya Mpingo wa ku Tiyatira (Chibvumbulutso 2:18-29) 
9. Kodi Mwapulumutsidwa mwa Madzi ndi Mzimu? 

MUTU 3
1. Kalata ya Mpingo wa ku Sarde (Chibuvumbulutso 3:1-6) 
2. Iwo Amene Sanadetse Zobvala Zao Zoyera 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Filadelfeya (Chibvumbulutso 3:7-13) 
4. Akapolo komanso Oyera Mtima a Mulungu Omwe Amakondweretsa Mtima Wake 
5. Kalata Ya Mpingo wa ku Laodikaya (Chibvumbulutso 3:14-22) 
6. Chikhulupiliro Choona cha Moyo wa Ophunzira 

MUTU 4
1. Onani Yesu Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu wa Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 
2. Yesu ndi Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 

MUTU 5 
1. Yesu Amene Waikidwa pa Mpando Wachifumu monga Woimilira wa Mulungu Atate (Chibvumbulutso 5:1-14) 
2. Mwanawankhosa Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu 

MUTU 6
1. Nyengo Zisanu ndi Ziwiri Zoikidwa ndi Mulungu (Chibvumbulutso 6:1-17) 
2. Nyengo za Zisindikizo Zisanu ndi Ziwiri 

MUTU 7
1. Ndindani Amene Adzapulumutsidwa mu Nthawi ya Chisautso Chachikulu? (Chibvumbulutso 7:1-17) 
2. Tiyeni Tikhale Ndi Chikhulupiliro Chomwe Chimamenya Nkhondo (Chibvumbuluitso 7:1-17) 
 
Chitapita chipolowe chazigewenga cha 9/11, mafunso ku “www.raptureready.com” Intaneti saiti pankhani ya nyengo, anachulukira kufika ku mamiliyoni opitilira ku 8 anafika, malinga ndi kafuku-fuku wa CNN ndi TIME, ma Ameleka opitilira pa 59% akhulupilira mkukwatula kosilizira.
Kunena za nyengo, mlembiyu akunena mfundo zeni-zeni za mutu wa buku la Chivumbulutso, kunenanso zakubwera kwa Wosusa Khristu, kuphedwa kwa oyera ndikukwatulidwa kwao, Ufumu wa zaka Chikwi chimodzi, ndi Kumwamba kwa Tsopano ndi Dziko la tsopano-zonse kulingana ndi Malembo wonse ndiponso motsogoleledwa ndi Mzimu Woyera.
Bukuli limapatsa ndemanga za ndime ndi ndime mu Buku la Chuvumbulutso powonjezedwa ndi ziphunzitso zozama za mlembi. Aliyense amene amawerenga bukuli adzadziwa zolinga zonse zimene Mulungu anasungira dzikoli lapansi.
Tsopano ndi nthawi kuti inu mdzindikire chofunikira cheni-cheni mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kotero kuti mupeze nzeru zimene zingakuomboleni kuchoka ku mayetsero onse ndi masautso a nthawi yamapeto. Ndi mabukuwa awiri, ndiponso pokhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, mdzakwanitsa kupambana mayetsero onse ndi masautso ananeneredwa mu Chivumbulutso.
Περισσότερα
Αναπαραγωγέας ηχητικού βιβλίου

Βιβλία που σχετίζονται με αυτόν τον τίτλο

The New Life Mission

Συμμετάσχετε στην έρευνά μας

Πώς μάθατε για εμάς;