• All e-books and audiobooks on The New Life Mission website are free
  • Explore multilingual sermons in global languages
  • Two new revised editions in English have been released
  • Check out our website translated into 27 languages
Search

FREE eBOOKS AND AUDIOBOOKS

The Gospel According to John

Chichewa  20

Ziphunzitso pa Uthenga wa Yohane (Ⅲ) - Idyani Mnofu Wanga Ndiponso Imwani Magazi Anga

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239771 | Pages 407

Download FREE eBook & AudioBook

Choose your preferred file format and safely download to your mobile device, PC, or tablet to read and listen to the sermon collections anytime, anywhere. All eBooks and AudioBooks are completely free.

You can listen to the AudioBook through the player below. 🔻
Own a Paperback
Buy a Paperback on Amazon
Zamkati 

Kalambulabwalo 
1. Kodi Mikate Yaying’noyi ndi Nsomba Ili ndi Nchito Yotani ku Anthu Ambiri (Yohane 6:1-15) 
2. Kukhulupilira mwa Iye Amene Mulungu Anasankha ndi Ntchito ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
3. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chokhalitsa Chopereka Moyo Wosatha (John 6:16-40) 
4. Kukhala Mogwirizana ndi Mzimu (Yohane 6:26-40) 
5. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chimene Sichikutha Padziko Lapansi (Yohane 6:26-59) 
6. Tiyenera Kudya Mkate Wochoka Kumwamba Mokhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu (Yohane 6:28-58) 
7. Yesu Khristu, Amene Anakhala Mkate wa Moyo kwa Ife (Yohane 6:41-51) 
8. Kodi Tingadye Bwanji Mnofu wa Yesu? (Yohane 6:41-59) 
9. Khulupilirani Mwa Yesu Amene Anachoka Kumwamba Ngati M’pulumutsi Wanu M’mtima Wanu (Yohane 6:41-51) 
10. Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Oona! (Yohane 6:47-51) 
11. Motengelako Mbali M’mgonero Oyera mwa Chikhulupiliro Choyenera (Yohane 6:52-59) 
12. Yesu, Amene Anatipatsa Mkate wa Umoyo (Yohane 6:54-63) 
13. Muyenera Kulalikira Mnofu ndi Magazi a Yesu ku Mamembala Abanja Lanu (Yohane 6:51-56) 
14. Cifukwa N’chiyani Tiyenera Kukhala ndi Moyo? (Yohane 6:63-69) 
15. Tiyenera Kukhala ndi Nzeru Yoyenera ya Choonadi (Yohane 6:60-71) 
 
Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Kupitira mu Mnofu Wake ndi Magazi

M’pingo ukusunga masakalamenti awiri olamulidwa ndi Yesu. Oyamba ndi ubatizo, ndipo wina ndi Mgonero Oyera. Tikutengako mbali mu Mgonero kuti tilingalire pa Choonadi cha uthenga chovumvulutsidwa mu mkate wake ndi mu vinyo, mwa kukumbukira uthengau.
Mu chiphikiro cha Mgonero Oyera, tikudya mkate mwa kukhumbukira mnofu wa Yesu, ndipo tikumwa vinyo ngati chiphikiro cha magazi Ake. mwakutero, tanthauzo lenileni la Mgonero Oyera ndi kulimbikitsa chikhulupiliro chathu mu Choonadi chakuti Yesu anatipulumutsa kumachimo adziko ndipo anatipatsa moyo osatha kupitira mu ubatizo Wake ndi imfa Yake pa Mtanda.
Koma, bvuto ndi lakuti pafupi-fupi Akristu onse akutengako mbali mu Mgonero Oyera mwachizolowezi, kopanda ngakhalenso kuzindikira cimene Yesu anatanthauza ndi mawu, “Mnofu Wanga ndi chakudwadi, ndipo magazi Anga ndi chakumwa chenicehni” (Yohane 6:55). Chotero, mkati mwa uthenga wa madzi ndi Mzimu, tikuyenera kulingaliranso pa tanthauzo la Yesu kutilamula kuti tidye mnofu Wake ndi kumwa magazi Ake, ndi kukhulupilira m’menemo.
More

Books related to this title

The New Life Mission

TAKE OUR SURVEY

How did you hear about us?