• All e-books and audiobooks on The New Life Mission website are free
  • Explore multilingual sermons in global languages
  • Two new revised editions in English have been released
  • Check out our website translated into 27 languages
Search

FREE eBOOKS AND AUDIOBOOKS

The Epistle of Paul the Apostle to the Ephesians

Chichewa  28

Chimene Mulungu Mtatu Anatichitira Ife - Ziphunzitso pa Aefeso (II)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240234 | Pages 442

Download FREE eBook & AudioBook

Choose your preferred file format and safely download to your mobile device, PC, or tablet to read and listen to the sermon collections anytime, anywhere. All eBooks and AudioBooks are completely free.

You can listen to the AudioBook through the player below. 🔻
Own a Paperback
Buy a Paperback on Amazon
Zamkati
 
Mawu Oyamba
1. Chipulumutso Chathu Chinakonzedwa Mu Chilungamo cha Yesu Ngakhalenso Pamene Dziko Lisanakhazikitsidwe (Aefeso 1:1-4) 
2. Takhala Akatundu a Mulungu mwa Chisomo Chake (Aefeso 1:1-14) 
3. Tinapulumutsidwa Kupitira mu Chikondi ndi Nsembe ya Mulungu (Aefeso 1:1-6) 
4. Tithokoza Mulungu Pakutiitana Ngati Mamembala a M’pingo Wake (Aefeso 1:20-23) 
5. Tili Ndichiombolo Mogwirizana Ndi Chuma cha Chisomo cha Mulungu (Aefeso 1:7-14) 
6. Kodi tinapangidwira Nchito Yolungama ya Ambuye? (Aefeso 2:1-10) 
7. Tiyenera Kudziwa Mphamvu ndi Chisomo cha Mulungu mu Umoyo Wathu Wachikhulupiliro (Aefeso 2:1-22) 
8. Kodi Tinali Mtundu wa Anthu Otani Pamaso pa Mulungu? (Aefeso 2:1-7) 
9. Takhala Osadziwika Kwa Mulungu Atate Cifukwa cha Machimo Athu (Aefeso 2:14-22) 
10. Madalitso Osaneneka a Khristu Ali M’mtima wa Oyera Aliyense Amene Akukhulupilira mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Aefeso 3:1-21) 
11. Tetezani Chikhulupiliro Chanu mu Umoyo Wanu (Aefeso 4:1-6) 
12. Tsanzirani Mulungu Ngati Ana Ake Okondedwa (Aefeso 5:1-2) 
13. Musatengeko Mbali Kumachimo Adziko (Aefeso 5:1-14) 
14. Kodi Kukhala mwa Kudzaza ndi Mzimu Chitanthauza Chiyani Kwenikweni? (Aefeso 5:1-21) 
15. Iwo Amene Akukhala mwa Kudzaza ndi Mzimu (Afeso 5:15-21) 
16. Tsutsanani ndi Machenjera a Satana (Aefeso 6:10-17) 
 
Kodi Mkudziwa M’mene Ulili M’pingo wa Mulungu?
 
Mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, muyenera kukhala ndi maso anu akuuzimu masiku onse otseguka. Ngati munalandira chikhululukiro cha machimo anu mwa kukhulupilira moona mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, ndiye kuti mdzatha kuzindikira M'pingo wa Mulungu moyenera; apo bii, simukanatha kudziwa moyenera imene ndi mipingo yaboza.
Masiku ano, Mulungu anakhazikitsa M'pingo Wake pachikhulupiliro cha okhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. M'pingo wa Mulungu ndi kusonkhana kwa aja amene anapulumutsidwa mwa kukhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Chotero, ngati mitima yanu tsopano ili ndi chikhulupiliro mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, ndiye kuti kenako mungakhale ndi chikhulupiliro mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kenako mungakhale moyo woona wachikhulupiliro. Moyo otero wachikhulupiliro ndi wotheka mu M'pingo wa Mulungu mokha. Moonjezera, chikhulupiliro chotere chokha chikutiyeneretsa kukakhala kwa muyaya mu Ufumu wa Ambuye. Kupitira muchikhulupiliro ichi, tiyenera kulandira chikondi cha chipulumutso ndi madalitso onse auzimu a Kumwamba kuchokera kwa Mulungu Atate, kwa Yesu Khristu, ndi ku Mzimu Woyera. 
More

Books related to this title

The New Life Mission

TAKE OUR SURVEY

How did you hear about us?