• 所有新生命宣教會 The New Life Mission 網站上的電子書和有聲書均可免費下載
  • 探索以多種語言提供的全球性講道
  • 查看我們已翻譯成27種語言的網站
  • 第1、2卷新修訂版已全新推出
Search

免費電子書和有聲讀物

使徒保羅寫給羅馬人的書信

奇切瓦語  6

Chilungamo cha Mulungu Chomwe Chaonetsedwa mu Aroma - Ambuye Wathu Yemwe Wakhala Chilungamo cha Mulungu (Ⅱ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 8983143215 | 頁碼 377

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
Zamkatimu
 
Mau Oyamba 

Mutu 7
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 7 
2. Mfundo ya Chikhulupiliro cha Paulo: Kulumikizana ndi Kristu titafa ku uchimo (Aroma 7:1-4) 
3. Chifukwa Chomwe Tingatamandire Ambuye (Aroma 7:5-13) 
4. Thupi lathu Lomwe Limatumikira Thupi Lokha Basi (Aroma 7:14-25) 
5. Thupi Limatumikira Lamulo la Uchimo (Aroma 7:24-25) 
6. Tamandani Ambuye, Mpulumutsi wa Ochimwa (Aroma 7:14-8:2) 

Mutu 8
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 8 
2. Chilungamo cha Mulungu, Chikwaniritso cha Chofunikira Cholungama cha Lamulo (Aroma 8:1-4) 
3. Kodi m’Kristu Ndindani? (Aroma 8:9-11) 
4. Chisamaliro cha Thupi chiri Imfa, koma Chisamaliro cha Mzimu chiri Moyo ndi Mtendere (Aroma 8:4-11) 
5. Kuyenda mu Chilungamo cha Mulungu (Aroma 8:12-16) 
6. Iwo amene amalowa Ufumu wa Mulungu (Aroma 8:16-27) 
7. Kubwera Kwachiwiri kwa Ambuye komanso Ufumu wa Zakachikwi (Aroma 8:18-25) 
8. Mzimu Woyera Umene Umathandiza Olungama (Aroma 8:26-28) 
9. Zinthu Zonse Zithandizana Kuwachitira Ubwino (Aroma 8:28-30) 
10. Ziphunzitso Zolakwika (Aroma 8:29-30) 
11. Chikondi Chosatha (Aroma 8:31-34) 
12. Ndindani Angayese Kutsutsana Nafe? (Aroma 8:31-34) 
13. Ndindani Amene Adzasiyanitsa Olungama ku Chikondi cha Kristu? (Aroma 8:35-39) 

Mutu 9
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 9 
2. Tiyenera Kudziwa Kuti Kukonzedweratu Kunakonzedwa Mkati mwa Chilungamo cha Mulungu (Aroma 9:9-33) 
3. Kodi ndi kulakwitsa Mulungu Kukonda Yakobo? (Aroma 9:30-33) 

Mutu 10
1. Mau Oyamba kwa Aroma Mutu 10 
2. Chikhulupiliro Chenicheni Chidza ndi Mbiri (Aroma 10:16-21) 

Mutu 11
1. Kodi Israyeli Adzapulumutsidwa? 

Mutu 12
1. Konzani Mtima Wanu Pamaso pa Mulungu 

Mutu 13
1. Khalani Chifukwa cha Chilungamo cha Mulungu 

Mutu 14
1. Musaweruzane Wina ndi Mnzake 

Mutu 15
1. Tiyeni Tifalitse Uthenga Wabwino ku Dziko Lonse Lapansi 

Mutu 16
1. Mulankhulane Wina ndi Mnzake 
 
Chilungamo Cha Mulungu chimaonekera ndipo chisiyana ndichija cha munthu. Chilungamo cha Mulungu chavumbulidwa muuthenga wamadzi ndi Mzimu, umene unakwaniritsidwa ndi kubadizidwa kwa Yesu kuli Yohane ndi mwazi Wake Pamtanda. Tibwerere kuchikhulupiliro cha Chilungamo cha Mulungu, tisachedwe.
Kodi ukudziwa ninji Yesu anabadizidwa ndi Yohne Mbadizi? Ngati Yohane sanabadize Yesu, machismo athu akanapatsidwa kwaiye. Yohane Mbadizi ndiye munthu wamkulu kupambana onse, ndipo ubadizo anapatsa Yesu unalingana ndichifuniro cha Mulungu kuti machismo athu apatsidwe kwa Yesu.
Yesu anabadizidwa kuti asenze machismo a anthu onse papewa pake, ndikufa pamtanda kulipa machismo. Zinthu zonsezi zasintha maganizo anga akuti kubadwanso nciani, chifukwa ndinangodziwa za mwazi pa Mtanda. Tsopano Mulungu wakupunzitsani kuti Chilungamo chake nhiani kuti tidziwe ndikukhulupilira mu Chilungamo chakecho mwatunthu. Ndithokoza Ambuye chifukwa chamadalitso onsewa.
更多
有聲書播放器

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?