• 所有新生命宣教會 The New Life Mission 網站上的電子書和有聲書均可免費下載
  • 探索以多種語言提供的全球性講道
  • 查看我們已翻譯成27種語言的網站
  • 第1、2卷新修訂版已全新推出
Search

免費電子書和有聲讀物

啟示錄

奇切瓦語  7

Ndemanga ndi Ulaliki pa Buku la Chibvumbulutso - KODI NYENGO YA WOTSUTSAKRISTU, KUFERA CHIKHULUPILIRO, MKWATULO KOMANSO UFUMU WA ZAKACHIKWI IKUDZA? ( I )

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928231294 | 頁碼 369

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
Zamkatimu 
 
Mau Oyamba 

MUTU 1
1. Imvani Mau a Chibvumbulutso cha Mulungu (Civumbulutso 1:1-20) 
2. Tiyenera Kudziwa Nyengo Zisanu Ndi Ziwiri 

MUTU 2
1. Kalata ya Mpingo wa ku Efeso (Chivumbulutso 2:1-7) 
2. Chikhulupiliro Chomwe Chingalandire Kuphedwa Chifukwa cha Kristu 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Smurna (Chibvumbuutso 2:8-11) 
4. Khalani Okhulupirika kufikira Imfa 
5. Ndindani Wopulumutsidwa ku Uchimo? 
6. Kalata ya Mpingo wa ku Pergamo (Chibvumbulutso 2:12-17) 
7. Osatira Chiphunzitso cha Anikolai 
8. Kalata ya Mpingo wa ku Tiyatira (Chibvumbulutso 2:18-29) 
9. Kodi Mwapulumutsidwa mwa Madzi ndi Mzimu? 

MUTU 3
1. Kalata ya Mpingo wa ku Sarde (Chibuvumbulutso 3:1-6) 
2. Iwo Amene Sanadetse Zobvala Zao Zoyera 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Filadelfeya (Chibvumbulutso 3:7-13) 
4. Akapolo komanso Oyera Mtima a Mulungu Omwe Amakondweretsa Mtima Wake 
5. Kalata Ya Mpingo wa ku Laodikaya (Chibvumbulutso 3:14-22) 
6. Chikhulupiliro Choona cha Moyo wa Ophunzira 

MUTU 4
1. Onani Yesu Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu wa Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 
2. Yesu ndi Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 

MUTU 5 
1. Yesu Amene Waikidwa pa Mpando Wachifumu monga Woimilira wa Mulungu Atate (Chibvumbulutso 5:1-14) 
2. Mwanawankhosa Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu 

MUTU 6
1. Nyengo Zisanu ndi Ziwiri Zoikidwa ndi Mulungu (Chibvumbulutso 6:1-17) 
2. Nyengo za Zisindikizo Zisanu ndi Ziwiri 

MUTU 7
1. Ndindani Amene Adzapulumutsidwa mu Nthawi ya Chisautso Chachikulu? (Chibvumbulutso 7:1-17) 
2. Tiyeni Tikhale Ndi Chikhulupiliro Chomwe Chimamenya Nkhondo (Chibvumbuluitso 7:1-17) 
 
Chitapita chipolowe chazigewenga cha 9/11, mafunso ku “www.raptureready.com” Intaneti saiti pankhani ya nyengo, anachulukira kufika ku mamiliyoni opitilira ku 8 anafika, malinga ndi kafuku-fuku wa CNN ndi TIME, ma Ameleka opitilira pa 59% akhulupilira mkukwatula kosilizira.
Kunena za nyengo, mlembiyu akunena mfundo zeni-zeni za mutu wa buku la Chivumbulutso, kunenanso zakubwera kwa Wosusa Khristu, kuphedwa kwa oyera ndikukwatulidwa kwao, Ufumu wa zaka Chikwi chimodzi, ndi Kumwamba kwa Tsopano ndi Dziko la tsopano-zonse kulingana ndi Malembo wonse ndiponso motsogoleledwa ndi Mzimu Woyera.
Bukuli limapatsa ndemanga za ndime ndi ndime mu Buku la Chuvumbulutso powonjezedwa ndi ziphunzitso zozama za mlembi. Aliyense amene amawerenga bukuli adzadziwa zolinga zonse zimene Mulungu anasungira dzikoli lapansi.
Tsopano ndi nthawi kuti inu mdzindikire chofunikira cheni-cheni mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kotero kuti mupeze nzeru zimene zingakuomboleni kuchoka ku mayetsero onse ndi masautso a nthawi yamapeto. Ndi mabukuwa awiri, ndiponso pokhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, mdzakwanitsa kupambana mayetsero onse ndi masautso ananeneredwa mu Chivumbulutso.
更多
有聲書播放器

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?