• 所有新生命宣教會 The New Life Mission 網站上的電子書和有聲書均可免費下載
  • 探索以多種語言提供的全球性講道
  • 查看我們已翻譯成27種語言的網站
  • 第1、2卷新修訂版已全新推出
Search

免費電子書和有聲讀物

約翰福音

奇切瓦語  20

Ziphunzitso pa Uthenga wa Yohane (Ⅲ) - Idyani Mnofu Wanga Ndiponso Imwani Magazi Anga

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239771 | 頁碼 407

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
Zamkati 

Kalambulabwalo 
1. Kodi Mikate Yaying’noyi ndi Nsomba Ili ndi Nchito Yotani ku Anthu Ambiri (Yohane 6:1-15) 
2. Kukhulupilira mwa Iye Amene Mulungu Anasankha ndi Ntchito ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
3. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chokhalitsa Chopereka Moyo Wosatha (John 6:16-40) 
4. Kukhala Mogwirizana ndi Mzimu (Yohane 6:26-40) 
5. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chimene Sichikutha Padziko Lapansi (Yohane 6:26-59) 
6. Tiyenera Kudya Mkate Wochoka Kumwamba Mokhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu (Yohane 6:28-58) 
7. Yesu Khristu, Amene Anakhala Mkate wa Moyo kwa Ife (Yohane 6:41-51) 
8. Kodi Tingadye Bwanji Mnofu wa Yesu? (Yohane 6:41-59) 
9. Khulupilirani Mwa Yesu Amene Anachoka Kumwamba Ngati M’pulumutsi Wanu M’mtima Wanu (Yohane 6:41-51) 
10. Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Oona! (Yohane 6:47-51) 
11. Motengelako Mbali M’mgonero Oyera mwa Chikhulupiliro Choyenera (Yohane 6:52-59) 
12. Yesu, Amene Anatipatsa Mkate wa Umoyo (Yohane 6:54-63) 
13. Muyenera Kulalikira Mnofu ndi Magazi a Yesu ku Mamembala Abanja Lanu (Yohane 6:51-56) 
14. Cifukwa N’chiyani Tiyenera Kukhala ndi Moyo? (Yohane 6:63-69) 
15. Tiyenera Kukhala ndi Nzeru Yoyenera ya Choonadi (Yohane 6:60-71) 
 
Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Kupitira mu Mnofu Wake ndi Magazi

M’pingo ukusunga masakalamenti awiri olamulidwa ndi Yesu. Oyamba ndi ubatizo, ndipo wina ndi Mgonero Oyera. Tikutengako mbali mu Mgonero kuti tilingalire pa Choonadi cha uthenga chovumvulutsidwa mu mkate wake ndi mu vinyo, mwa kukumbukira uthengau.
Mu chiphikiro cha Mgonero Oyera, tikudya mkate mwa kukhumbukira mnofu wa Yesu, ndipo tikumwa vinyo ngati chiphikiro cha magazi Ake. mwakutero, tanthauzo lenileni la Mgonero Oyera ndi kulimbikitsa chikhulupiliro chathu mu Choonadi chakuti Yesu anatipulumutsa kumachimo adziko ndipo anatipatsa moyo osatha kupitira mu ubatizo Wake ndi imfa Yake pa Mtanda.
Koma, bvuto ndi lakuti pafupi-fupi Akristu onse akutengako mbali mu Mgonero Oyera mwachizolowezi, kopanda ngakhalenso kuzindikira cimene Yesu anatanthauza ndi mawu, “Mnofu Wanga ndi chakudwadi, ndipo magazi Anga ndi chakumwa chenicehni” (Yohane 6:55). Chotero, mkati mwa uthenga wa madzi ndi Mzimu, tikuyenera kulingaliranso pa tanthauzo la Yesu kutilamula kuti tidye mnofu Wake ndi kumwa magazi Ake, ndi kukhulupilira m’menemo.
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?