• 所有新生命宣教會 The New Life Mission 網站上的電子書和有聲書均可免費下載
  • 探索以多種語言提供的全球性講道
  • 查看我們已翻譯成27種語言的網站
  • 第1、2卷新修訂版已全新推出
Search

免費電子書和有聲讀物

創世記

奇切瓦語  23

Ziphunzitso pa Genesis (Ⅱ) - Kugwa kwa Munthu ndi Chipulumutso Cholungama cha Mulungu

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928240050 | 頁碼 362

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
Zamkati
 
Kalambulabwalo

CHAPITALA 2
1. Madalitso Amene Mulungu Anatipatsa (Genesis 2:1-3) 
2. Maganizo a Munthu Ali Ngati Nkhungu (Genesis 2:4-6) 
3. Tinakumana ndi Yesu Khristu Mkwati Wathu (Genesis 2:21-25) 

CHAPITALA 3
1. Choonadi Sichisintha Ngakhale Anthu Ambiri Angachikane Motani (Genesis 3:1-4) 
2. Uchimo Unadzalowa Mdzikoli (Genesis 3:1-6) 
3. Kodi Chikhulupiliro Chathu Tiyenera Kuimilika Poti? (Genesis 3:1-7) 
4. Mphamvu ya Chikhulupiliro mwa Mulungu (Genesis 3:1-7) 
5. Tingagonjetse Satana mwa Chikhulupiliro Choona Chokha (Genesis 3:1-7) 
6. Tiyenera Kugonjetsa Chinyengo cha Satana Mwa Kukhulupilira mu Uthenga Oona (Genesis 3:1-7) 
7. Masiku Onse Funani Chophindulira Mulungu Chokha (Genesis 3:1-24) 
8. Machimo Athu Anatsukidwa Mwakukhulupilira mu Uthenga Weniweni (Genesis 3:8-10) 
9. Tiyenera Kukhala ndi Moyo Malinga ndi Zokhumba za Mzimu Woyera (Genesis 3:8-17) 
10. Kodi Chabwino Chenicheni Ndi Choipa Chenicheni N’chiyani? (Genesis 3:10-24) 
11. Chisamaliro cha Mulungu (Genesis 3:13-24) 
12. Kodi Tiyenera Kukhala ndi Moyo Mwa Ndani? (Genesis 3:17-21) 
 
Mu Buku la Genesisi, cholinga cha cimene Mulungu anatilengera chipezeza. Pamene architekicha alemba nyumba kapena wolemba adinda chithunzi, poyamba amayamba akhala ndi nchito ija imene angakwanilitsidwe mu maganizo yawo sanayambe kugwira nchito pa polonjekiti yawo. Monga chotero, Mulungu nayenso anali ndi chipulumutso chathu mu maganizo Ake ngakhale Iye asanalenge kumwamba ndi dziko lapansi, ndipo anapanga Adamu ndi Hava mu cholinga Chake cha mu maganizo. Ndipo Mulungu anafotokoza za malo a Kumwamba, amene samaoneka ndi maso athu a thupi, polemba mndandanda wa malo apadziko lapansi amene tingayaone tonse ndi kumvesetsa.
Ngakhale kuchokera pamaziko ya dziko, Mulungu anali kufuna kupulumutsa anthu molungama popereka uthenga wa madzi ndi Mzimu ku mtima wa aliyense. Kotero ngakhale anthu onse anapangidwa kuchokera kufumbi, ayenera kuphunzira ndi kudziwa Choonadi cha uthenga wa madzi ndi Mzimu kuti miyoyo yawo yisangalale. Anthu akapitiriza kukhala opanda kudzindikira mphamvu za Kumwamba, adzataya zinthu osati za padziko lapansi zokha, komaso ndi zonse za Kumwamba.
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?