• 所有新生命宣教會 The New Life Mission 網站上的電子書和有聲書均可免費下載
  • 探索以多種語言提供的全球性講道
  • 查看我們已翻譯成27種語言的網站
  • 第1、2卷新修訂版已全新推出
Search

免費電子書和有聲讀物

異教徒

奇切瓦語  25

Ampatuko, Amene Anasatira Machimo a YEROBOWAMU (I)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928241774 | 頁碼 332

下載免費電子書和有聲讀物

選擇您喜歡的文件格式,安全下載到手機、電腦或平板電腦,隨時隨地閱讀和收聽講道集。所有電子書和有聲讀物都完全免費。

您可以通過下方播放器收聽有聲讀物。🔻
擁有平裝書
在亞馬遜購買平裝書
Zamkati
 
Kalambulabwalo
1. Kodi Ampatuko ndi Otani Pamaso pa Mulungu? (1 Mafumu 11:1-13) 
2. Kodi Akristu Amene Akhulupilira Mwa Yesu Mkati mwa Chikonzero cha Nchito Yochokera Mkuganiza kwa Kuthupi Kwawo ndi Otani? (1 Mafumu 12:25-33) 
3. Kutsatira Zokhumba za Thupi Kuzakupangitsa kukhala Wampatuko Nthawi Imeneyo (1 Mafumu 12:1-18) 
4. Kodi ndi mu Uthenga Otani mu Umene Tsopano Mkukhulupilira? (1 Mafumu 13:33-34) 
5. Akristu a Masiku Ano Amene Anachosapo Mulungu N’kuikapo Zinthu Zopanda Pake ndi Opembeza Mafano Pamaso pa Mulungu (1 Mafumu 11:1-13) 
6. Kodi Mulungu Akupulumutsa Bwanji Ampatuko? (1 Mafumu 19:1-21) 
7. Muyenera Kukhulupilira Kuti Yohane M’batizi ndi Oimilirako Anthu Onse (Mateyu 11:1-19) 
8. Mitundu 7 ya Anthu Amene Adzatembeleledwa ndi Mulungu (Mateyu 23:1-36) 
9. Chilitsani Madzi Oipa ndi Mchere (2 Mafumu 2:19-22) 
 
Mu Baibulo, anthu a Isiraeli akunena kuti akupembeza Mulungu, koma pamapeto ake, anasatira Yerobowamu, anali kupembeza ana ang’ombe agolide. Mchoona, kopitila 2/3 ya mbiri ya Aisiraeli inali mbiri yakupembeza ana ang’ombe agolide, kuganiza kuti iwo ndi Mulungu. Pothera pake, ngakhalenso tsopanoli, akupitiliza kukhala ndi moyo kopanda kuzindikira choona kuti Yesu Khristu, amene anabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kuti ndi M’pulumutsi wawo oona. Kosasamala za ichi, kuli aYuda ambiri amene akuyembekezera za M’pulumutsi wawo, ngakhalenso tsopanoli. 
Kodi ndiyeno, chikhulupiliro chanu inu amene mkunena kuti mkutengako mbali mu Chikristu Mnthawiyi ya Chipangano cha Tsopano chii motani? Kodi tsopano mkukhulupilira mu ndi kusatira Mulungu mwakumvetsetsa koyenera kwa Iye? Ngati ai, kodi mwina mwake inu si mkupembeza ana ang’ombe agolide mwakusamvetsetsa iwo ngati Mulungu? Ngati muli choncho, ndiye kuti muyenera kudziwa za choona chakuti mkupembeza fano pamaso pa Mulungu ngati anthu a Isiraeli. Ndiye kuti, muyenera kubweleranso ndi kukumana ndi Ambuye amene anabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu. Ndikhulupilira kuti mdzakwanitsa kukhulupilira mu Choonadi ngati mwazindikiradi pamaso pa Mulungu cimene ndi Choonadi cha chipulumutso mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kodi si mdzatero? 
Ndifuna kuchitira umboni pamaso pa inu chikhulupiliro choona ndi Choonadi pa chapamutu, “Ampatuko, Amene anasatira machimo a Yerobowamu.” Mwanjira zonse, Ndikhulupilira mdzakhala anthu a chikhulupiliro chofanana ngati chija changa. 
更多

與該標題相關的書籍

The New Life Mission

參加我們的調查

您是如何得知我們的?