Search

DARMOWE E-BOOKI I AUDIOBOOKI

List Apostoła Pawła do Galacjan

Cziczewa  16

Ziphunzitso mu Agalatiya - Kuchoka Kumdulidwe wa Kuthupi Kufika Kuchiphunzitso Cha Kulapa (Ⅰ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239474 | Strony 463

Pobierz e-booki i audiobooki ZA DARMO

Wybierz preferowany format pliku i bezpiecznie pobierz na telefon komórkowy, komputer lub tablet, aby czytać i słuchać kolekcji kazań w dowolnym miejscu i czasie. Wszystkie e-booki i audiobooki są całkowicie bezpłatne.

Możesz słuchać audiobooka przez odtwarzacz poniżej. 🔻
Posiadaj książkę w miękkiej oprawie
Kup książkę w miękkiej oprawie na Amazon
Zamkati
 
Kalambulabwalo 

CHAPITALA 1
1. Ambuye Anatilanditsa Kudzikoli Loipa (Galatiya 1:1-5) 
2. Kodi Chikhulupiliro Chanu Sichili Chofanana ndi Cha Amudulidwe Mwina? (Galatiya 1:1-5) 
3. Ambuye Anatilanditsa Mwa Ungwiro ndiponso Mwa Kamodzi Kokha (Galatiya 1:3-5) 
4. Sipangakhalenso Uthenga Wina Koma Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 1:6-10) 
5. Aja Amene Mitima Yawo Inaikidwa Ngati Atumiki a Mulungu (Galatiya 1:10-12) 
6. Chikhulupiliro Cha Mtumwi Paulo Ndi Chenjezo Lake ku Amudulidwe (Galatiya 1:1-17) 
7. Moyo Wachikhulupiriro Chachilamulo Ubweretsa Matemberero Okha (Galatiya 1:1-24) 

CHAPITALA 2
1. Chifukwa N’chiyani Mtumwi Paulo Anasura a Zachilamulo? (Galatiya 2:1-10) 
2. Tanthauzo Leni-leni la Chikhulupiliro cha Paulo (Galatiya 2:20) 
3. Mwachikhulupiliro mu Mwana wa Mulungu, Kodi Tinafa ndi Kuukitsidwa Limodzi Ndi Iye? (Galatiya 2:20) 
4. Munthu Samayetsedwa Olungama ndi Nchito za Chilamulo Koma mwa Chikhulupiliro mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 2:11-21) 
5. Tikuyetsedwa Wolungama mwa Chikhulupiliro Choyera Chokha (Galatiya 2:11-21) 

CHAPITALA 3
1. Masiku Onse Khalani Moyo wanu Mwa Chikhulupiliro mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Galatiya 3:1-11) 
2. Kodi Kupanda Kanthu kwa Mitima Yathu Kukuzimiririka Nthawi Yotani? (Galatiya 3:23-29) 
3. Tsopano Sitiyenera Kukhalanso Pansi pa Matembelelo a Chilamulo (Galatiya 3:1-29) 
 
Chiphunzitso cha Kulapa Ndichokwanira Kukupanhitsani kuti Mtore Matenda a Kuuzimu.

Anthu mdziko lonse ali ndi mantha ndi tudoyo ngati SARS, cifukwa angafe mwamusanga mwa kuonetsedwa ku tudoyo totero tosaoneka.
Chimodzimodzi, Akristu masiku ano kudzungulira dziko lonse akufa mu mathupi awo ndiponso mu mzimu mwa kudwara ndi chiphunzitso cha kulapa. Kodi munali kudziwa kuti chiphunzitso cha kulapa ndi cholakwika moteromu?
Kodi mkudziwa amene anapangitsa Akristu kugwera mu dzenje lolowelera la chisokonezo cha mu mzimu. Ndi Akristu ochimwa iwo okha amene akupemphera mapemphero akulapa tsiku ndi tsiku kuti ayeretsedwe kumachimo awo a payekha payekha pamene akunena kuti okhulupilira mwa Yesu Khristu ngati M’pulumutsi wawo.
Chotero, muyenera kulandira chikhululukiro cha machimo mwa kukhulupilira mu Mawu a uthenga wa madzi ndi Mzimu umene Mulungu anatipatsa pachiyambi. Si muyenera kutaya mpata odalitsidwa okhala obadwa mwatsopano. Tonsefe tiyenera kumasulidwa kuchisokonezo cha mu mzimu mwa kukhulupilira mu Choonadi cha uthenga wa madzi ndi Mzimu. Tiyenera kuyangana pa kuwala konyezimira kwa Choonadi, cimene chinabwera kudzera mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, titathawako kunjira ya chisokonezo cha mu mzimu.
Więcej

Książki związane z tym tematem

The New Life Mission

Weź udział w naszej ankiecie

Skąd się o nas dowiedziałeś?