Search

DARMOWE E-BOOKI I AUDIOBOOKI

Ewangelia Według Jana

Cziczewa  20

Ziphunzitso pa Uthenga wa Yohane (Ⅲ) - Idyani Mnofu Wanga Ndiponso Imwani Magazi Anga

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239771 | Strony 407

Pobierz e-booki i audiobooki ZA DARMO

Wybierz preferowany format pliku i bezpiecznie pobierz na telefon komórkowy, komputer lub tablet, aby czytać i słuchać kolekcji kazań w dowolnym miejscu i czasie. Wszystkie e-booki i audiobooki są całkowicie bezpłatne.

Możesz słuchać audiobooka przez odtwarzacz poniżej. 🔻
Posiadaj książkę w miękkiej oprawie
Kup książkę w miękkiej oprawie na Amazon
Zamkati 

Kalambulabwalo 
1. Kodi Mikate Yaying’noyi ndi Nsomba Ili ndi Nchito Yotani ku Anthu Ambiri (Yohane 6:1-15) 
2. Kukhulupilira mwa Iye Amene Mulungu Anasankha ndi Ntchito ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
3. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chokhalitsa Chopereka Moyo Wosatha (John 6:16-40) 
4. Kukhala Mogwirizana ndi Mzimu (Yohane 6:26-40) 
5. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chimene Sichikutha Padziko Lapansi (Yohane 6:26-59) 
6. Tiyenera Kudya Mkate Wochoka Kumwamba Mokhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu (Yohane 6:28-58) 
7. Yesu Khristu, Amene Anakhala Mkate wa Moyo kwa Ife (Yohane 6:41-51) 
8. Kodi Tingadye Bwanji Mnofu wa Yesu? (Yohane 6:41-59) 
9. Khulupilirani Mwa Yesu Amene Anachoka Kumwamba Ngati M’pulumutsi Wanu M’mtima Wanu (Yohane 6:41-51) 
10. Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Oona! (Yohane 6:47-51) 
11. Motengelako Mbali M’mgonero Oyera mwa Chikhulupiliro Choyenera (Yohane 6:52-59) 
12. Yesu, Amene Anatipatsa Mkate wa Umoyo (Yohane 6:54-63) 
13. Muyenera Kulalikira Mnofu ndi Magazi a Yesu ku Mamembala Abanja Lanu (Yohane 6:51-56) 
14. Cifukwa N’chiyani Tiyenera Kukhala ndi Moyo? (Yohane 6:63-69) 
15. Tiyenera Kukhala ndi Nzeru Yoyenera ya Choonadi (Yohane 6:60-71) 
 
Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Kupitira mu Mnofu Wake ndi Magazi

M’pingo ukusunga masakalamenti awiri olamulidwa ndi Yesu. Oyamba ndi ubatizo, ndipo wina ndi Mgonero Oyera. Tikutengako mbali mu Mgonero kuti tilingalire pa Choonadi cha uthenga chovumvulutsidwa mu mkate wake ndi mu vinyo, mwa kukumbukira uthengau.
Mu chiphikiro cha Mgonero Oyera, tikudya mkate mwa kukhumbukira mnofu wa Yesu, ndipo tikumwa vinyo ngati chiphikiro cha magazi Ake. mwakutero, tanthauzo lenileni la Mgonero Oyera ndi kulimbikitsa chikhulupiliro chathu mu Choonadi chakuti Yesu anatipulumutsa kumachimo adziko ndipo anatipatsa moyo osatha kupitira mu ubatizo Wake ndi imfa Yake pa Mtanda.
Koma, bvuto ndi lakuti pafupi-fupi Akristu onse akutengako mbali mu Mgonero Oyera mwachizolowezi, kopanda ngakhalenso kuzindikira cimene Yesu anatanthauza ndi mawu, “Mnofu Wanga ndi chakudwadi, ndipo magazi Anga ndi chakumwa chenicehni” (Yohane 6:55). Chotero, mkati mwa uthenga wa madzi ndi Mzimu, tikuyenera kulingaliranso pa tanthauzo la Yesu kutilamula kuti tidye mnofu Wake ndi kumwa magazi Ake, ndi kukhulupilira m’menemo.
Więcej

Książki związane z tym tematem

The New Life Mission

Weź udział w naszej ankiecie

Skąd się o nas dowiedziałeś?