Search

ספרים אלקטרוניים וספרי אודיו חינמיים

הבשורה על פי מתי

צ\\\'יצ\\\'ווה  13

ULALIKI PA UTHENGA WABWINO WA MATEYU (II) - KODI TINAKHULUPIRIRA CHIYANI KUTI TILANDIRE CHIKHULULUKIRO CHA MACHIMO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928260089 | עמודים 512

חינם הורד ספרים אלקטרוניים וספרי שמע

בחר את תבנית הקובץ המועדפת עליך והורד בבטחה למכשיר הנייד, המחשב או הטאבלט שלך כדי לקרוא ולהאזין לאוספי הדרשות בכל זמן ומקום. כל הספרים האלקטרוניים וספרי השמע ניתנים לחלוטין בחינם.

🔻ניתן להאזין לספר השמע באמצעות הנגן שלמטה.
היה בעלים של ספר בכריכה רכה
קנה ספר בכריכה רכה באמזון
Zamkatimu 
 
Mau Oyamba 

MUTU 9
1. Khulupilirani mwa Yesu Kristu Yemwe Anadza Monga Mulungu Wathu (Mateyu 9:1-13) 
2 .Yesu Yemwe Anadza Kudzapulumutsa Ife, Amanjenje Auzimu (Mateyu 9:1-13) 
3. Chikhulupiliro cha Chipembedzo Motsutsana ndi Chikhulupiliro mu Mphamvu ya Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu (Mateyu 9:1-13) 
4. Antchito a Mulungu (Mateyu 9:35-38) 

MUTU 10
1. Mphamvu Yochiritsa Matenda Onse Imapezeka mu Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Mateyu 10:1-16) 
2. Tiyeni Tikhale Monga Antchito a Mulungu (Mateyu 10:1-8) 

MUTU 11
1. Yohane Mbatizi Sanali Wolephera (Mateyu 11:1-14) 

MUTU 12
1. Yesu Ananena Kuti Iye Amafuna Chifundo Osati Nsembe (Mateyu 12:1-8) 
2. Kodi Mukufuna Kudziwa Kuti Kuchitira Mwano Mzimu Woyera ndi Chiani? (Mateyu 12:9-37) 
3. Tchimo Losakhululukidwa komaso Ntchito ya Obadwa Mwatsopano (Mateyu 12:31-32)
4. Kodi Satana Amafuna Kukhala Kuti? (Mateyu 12:43-50) 

MUTU 13 
1. Fanizo la Mitundu Inayi ya Minda (Mateyu 13:1-9) 
2. Inu Mwaloledwa Kudziwa Zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba (Mateyu 13:10-23) 
3. Ufumu wa Kumwamba Ufanizidwa ndi Munthu, Amene Anafesa Mbeu Zabwino M’munda Mwace (Mateyu 13:24-30) 
4. Mphamvu ya Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu (Mateyu 13:31-43) 
5. Ufumu wa Kumwamba Uli Wofanana ndi Cuma Cobisika M’munda (Mateyu 13:44-46)
6. Ufumu wa Kumwamba Uli Wofanana ndi Khoka Loponyedwa m’Nyanja Ndi Kusonkhanitsa Pamodzi Za Mitundu Yonse (Mateyu 13:47-52) 
7. Mariya Ndithudi Si Waumulungu (Mateyu 13:53-58)
 
Mtumwi Mateyu akutiuza ife kuti Mau a Yesu analankhulidwa kwa aliyense m’dziko lino, popeza Iye ankaona Yesu monga Mfumu ya mafumu. Tsopano, Akristu dziko lonse lapansi, amene angobadwa mwatsopano pokhulupilira mu uthenga wabwino wa madzi ndi Mzimu omwe tikufalitsa, indedi akufunitsitsa kudya mkate wamoyo. Koma ndikobvuta kwa iwo kukhala ndi chiyanjano ndi ife mu uthenga wabwino weni weni, popeza iwo onse ali kutali ndi ife. Choncho, kuti tikumane ndi zofunika zauzimu za anthu amenewa a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ulaliki m’buku limeneli wakonzedwa monga mkate watsopano wa moyo kwa iwo kuti usamalire kukula kwao kwauzimu. Mlembi amanena kuti iwo amene alandira chikhululukiro cha machimo ao pokhulupilira m’Mau a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ayenera kudya Mau Ake angwiro pofuna kuteteza chikhulupiliro chao komanso kuchita bwino m’miyoyo yao yauzimu. Buku limeneli lidzapereka mkate weni weni wamoyo wauzimu kwa inu nonse amene mwakhala anthu olemekezeka a Mfumu mwa chikhulupiliro. Kudzera mu Mpingo Wake ndi akapolo Ake, Mulungu adzapitiriza kupereka kwa inu mkate umenewu wamoyo. Lolani madalitso a Mulungu akhale pa inu nonse amene mwabadwa mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu, amene mukufuna kukhala ndi chiayanjano chauzimu ndi ife mwa Yesu Kristu.
עוד
ספר מודפס בחינם
הוסף ספרים לעגלה.
נגן ספרים מוקלטים

ספרים הקשורים לכותר זה

The New Life Mission

השתתף בסקר שלנו

איך שמעת עלינו?