Search

SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Khải huyền

Tiếng Chichewa  7

Ndemanga ndi Ulaliki pa Buku la Chibvumbulutso - KODI NYENGO YA WOTSUTSAKRISTU, KUFERA CHIKHULUPILIRO, MKWATULO KOMANSO UFUMU WA ZAKACHIKWI IKUDZA? ( I )

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928231294 | Trang 369

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkatimu 
 
Mau Oyamba 

MUTU 1
1. Imvani Mau a Chibvumbulutso cha Mulungu (Civumbulutso 1:1-20) 
2. Tiyenera Kudziwa Nyengo Zisanu Ndi Ziwiri 

MUTU 2
1. Kalata ya Mpingo wa ku Efeso (Chivumbulutso 2:1-7) 
2. Chikhulupiliro Chomwe Chingalandire Kuphedwa Chifukwa cha Kristu 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Smurna (Chibvumbuutso 2:8-11) 
4. Khalani Okhulupirika kufikira Imfa 
5. Ndindani Wopulumutsidwa ku Uchimo? 
6. Kalata ya Mpingo wa ku Pergamo (Chibvumbulutso 2:12-17) 
7. Osatira Chiphunzitso cha Anikolai 
8. Kalata ya Mpingo wa ku Tiyatira (Chibvumbulutso 2:18-29) 
9. Kodi Mwapulumutsidwa mwa Madzi ndi Mzimu? 

MUTU 3
1. Kalata ya Mpingo wa ku Sarde (Chibuvumbulutso 3:1-6) 
2. Iwo Amene Sanadetse Zobvala Zao Zoyera 
3. Kalata ya Mpingo wa ku Filadelfeya (Chibvumbulutso 3:7-13) 
4. Akapolo komanso Oyera Mtima a Mulungu Omwe Amakondweretsa Mtima Wake 
5. Kalata Ya Mpingo wa ku Laodikaya (Chibvumbulutso 3:14-22) 
6. Chikhulupiliro Choona cha Moyo wa Ophunzira 

MUTU 4
1. Onani Yesu Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu wa Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 
2. Yesu ndi Mulungu (Chibvumbulutso 4:1-11) 

MUTU 5 
1. Yesu Amene Waikidwa pa Mpando Wachifumu monga Woimilira wa Mulungu Atate (Chibvumbulutso 5:1-14) 
2. Mwanawankhosa Yemwe Wakhala pa Mpando Wachifumu 

MUTU 6
1. Nyengo Zisanu ndi Ziwiri Zoikidwa ndi Mulungu (Chibvumbulutso 6:1-17) 
2. Nyengo za Zisindikizo Zisanu ndi Ziwiri 

MUTU 7
1. Ndindani Amene Adzapulumutsidwa mu Nthawi ya Chisautso Chachikulu? (Chibvumbulutso 7:1-17) 
2. Tiyeni Tikhale Ndi Chikhulupiliro Chomwe Chimamenya Nkhondo (Chibvumbuluitso 7:1-17) 
 
Chitapita chipolowe chazigewenga cha 9/11, mafunso ku “www.raptureready.com” Intaneti saiti pankhani ya nyengo, anachulukira kufika ku mamiliyoni opitilira ku 8 anafika, malinga ndi kafuku-fuku wa CNN ndi TIME, ma Ameleka opitilira pa 59% akhulupilira mkukwatula kosilizira.
Kunena za nyengo, mlembiyu akunena mfundo zeni-zeni za mutu wa buku la Chivumbulutso, kunenanso zakubwera kwa Wosusa Khristu, kuphedwa kwa oyera ndikukwatulidwa kwao, Ufumu wa zaka Chikwi chimodzi, ndi Kumwamba kwa Tsopano ndi Dziko la tsopano-zonse kulingana ndi Malembo wonse ndiponso motsogoleledwa ndi Mzimu Woyera.
Bukuli limapatsa ndemanga za ndime ndi ndime mu Buku la Chuvumbulutso powonjezedwa ndi ziphunzitso zozama za mlembi. Aliyense amene amawerenga bukuli adzadziwa zolinga zonse zimene Mulungu anasungira dzikoli lapansi.
Tsopano ndi nthawi kuti inu mdzindikire chofunikira cheni-cheni mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, kotero kuti mupeze nzeru zimene zingakuomboleni kuchoka ku mayetsero onse ndi masautso a nthawi yamapeto. Ndi mabukuwa awiri, ndiponso pokhulupilira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu, mdzakwanitsa kupambana mayetsero onse ndi masautso ananeneredwa mu Chivumbulutso.
Thêm
Trình phát sách nói

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?