Search

SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Phúc-âm theo Ma-thi-ơ

Tiếng Chichewa  12

ULALIKI PA UTHENGA WABWINO WA MATEYU (I) - KODI NDIPATI PAMENE M’KRISTU ANGATHE KUKHALA NDI KUKAMBIRANA KWA PAMTIMA NDI AMBUYE?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928238859 | Trang 406

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkatimu 

Mau Oyamba 

MUTU 1
1. Mbadwo wa Yesu Kristu (Mateyu 1:1-6) 
2. Tiyeni Tiyamike Ambuye Wanthu Amene Anabwera Kudzatipulumutsa Ife (Mateyu 1:18-25) 
3. Yesu Amene Anabadwa Mwa Mzimu Woyera (Mateyu 1:18-25) 

MUTU 2
1. Kodi Tingakumane Kuti ndi Ambuye Moyenera? (Mateyu 2:1-12)

MUTU 3
1. Kufalitsa Uthenga Wabwino Oona Ndi Ntchito Yolungama Ya Yesu (Mateyu 3:1-17) 
2. Yesu Amene Anabwera Kuti Afafanize Machimo Anu (Mateyu 3:13-17) 

MUTU 4
1. Dalitso Ndi Kuopa Mulungu ndi Kutumikira Mulungu (Mateyu 4:1-11) 

MUTU 5 
1. Ulaliki pa Phiri (Mateyu 5:1-16)

MUTU 6
1. Chiphunzitso cha Ambuye pa Pemphero (1) (Mateyu 6:1-15) 
2. Chiphunzitso cha Ambuye pa Pemphero (2) (Mateyu 6:5-15) 
3. Khalani ndi Mitima Yanu pa Ambuye (Mateyu 6:21-23)
4. Musadere Nkhawa za Moyo Wanu, Koma Dalirani mwa Mulungu Yekha (Mateyu 6:25-34) 
5. Zikwanire Tsiku Zobvuta Zake (Mateyu 6:34) 

MUTU 7
1. Pokhulupilira mu Mphamvu ya Uthenga Wabwino, Tiyenera Kulowa Kudzera mu Cipata Copapatiza (Mateyu 7:13-14) 
2. Kodi Tidzachita Chiani Ngati Tidzakanidwa ndi Ambuye pa Tsiku Lotsiriza? (Mateyu 7:21-23) 
3. Chikhulupiliro Chomwe Chingathe Kuchita Chifuniro cha Mulungu Atate (Mateyu 7:20-27) 
4. Tingathe Kulowa Kumwamba Pokhapo Ngati Tadziwa Chifuniro cha Atate ndi Kukhulupilira mu Icho (Mateyu 7:21-27) 
5. Chenjerani ndi Aneneri Onyega Omwe Amangofuna Ndalama Zanu (Mateyu 7:13-27) 

MUTU 8
1. Machiritso a Akhate Auzimu (Mateyu 8:1-4) 
2. “Mungonena Mau” (Mateyu 8:5-10) 
3. Tsatani Ambuye Poyamba (Mateyu 8:18-22) 

Mtumwi Mateyu akutiuza ife kuti Mau a Yesu analankhulidwa kwa aliyense m’dziko lino, popeza Iye ankaona Yesu monga Mfumu ya mafumu. Tsopano, Akristu dziko lonse lapansi, amene angobadwa mwatsopano pokhulupilira mu uthenga wabwino wa madzi ndi Mzimu omwe tikufalitsa, indedi akufunitsitsa kudya mkate wamoyo. Koma ndikobvuta kwa iwo kukhala ndi chiyanjano ndi ife mu uthenga wabwino weni weni, popeza iwo onse ali kutali ndi ife. Choncho, kuti tikumane ndi zofunika zauzimu za anthu amenewa a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ulaliki m’buku limeneli wakonzedwa monga mkate watsopano wa moyo kwa iwo kuti usamalire kukula kwao kwauzimu. Mlembi amanena kuti iwo amene alandira chikhululukiro cha machimo ao pokhulupilira m’Mau a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ayenera kudya Mau Ake angwiro pofuna kuteteza chikhulupiliro chao komanso kuchita bwino m’miyoyo yao yauzimu. Buku limeneli lidzapereka mkate weni weni wamoyo wauzimu kwa inu nonse amene mwakhala anthu olemekezeka a Mfumu mwa chikhulupiliro. Kudzera mu Mpingo Wake ndi akapolo Ake, Mulungu adzapitiriza kupereka kwa inu mkate umenewu wamoyo. Lolani madalitso a Mulungu akhale pa inu nonse amene mwabadwa mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu, amene mukufuna kukhala ndi chiayanjano chauzimu ndi ife mwa Yesu Kristu.
Thêm
Trình phát sách nói

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?