Search

SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Phúc-âm Giăng

Tiếng Chichewa  20

Ziphunzitso pa Uthenga wa Yohane (Ⅲ) - Idyani Mnofu Wanga Ndiponso Imwani Magazi Anga

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239771 | Trang 407

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkati 

Kalambulabwalo 
1. Kodi Mikate Yaying’noyi ndi Nsomba Ili ndi Nchito Yotani ku Anthu Ambiri (Yohane 6:1-15) 
2. Kukhulupilira mwa Iye Amene Mulungu Anasankha ndi Ntchito ya Mulungu (Yohane 6:16-29) 
3. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chokhalitsa Chopereka Moyo Wosatha (John 6:16-40) 
4. Kukhala Mogwirizana ndi Mzimu (Yohane 6:26-40) 
5. Gwirani Ntchito ya Chakudya Chimene Sichikutha Padziko Lapansi (Yohane 6:26-59) 
6. Tiyenera Kudya Mkate Wochoka Kumwamba Mokhulupilira mu Uthenga wa madzi ndi Mzimu (Yohane 6:28-58) 
7. Yesu Khristu, Amene Anakhala Mkate wa Moyo kwa Ife (Yohane 6:41-51) 
8. Kodi Tingadye Bwanji Mnofu wa Yesu? (Yohane 6:41-59) 
9. Khulupilirani Mwa Yesu Amene Anachoka Kumwamba Ngati M’pulumutsi Wanu M’mtima Wanu (Yohane 6:41-51) 
10. Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Oona! (Yohane 6:47-51) 
11. Motengelako Mbali M’mgonero Oyera mwa Chikhulupiliro Choyenera (Yohane 6:52-59) 
12. Yesu, Amene Anatipatsa Mkate wa Umoyo (Yohane 6:54-63) 
13. Muyenera Kulalikira Mnofu ndi Magazi a Yesu ku Mamembala Abanja Lanu (Yohane 6:51-56) 
14. Cifukwa N’chiyani Tiyenera Kukhala ndi Moyo? (Yohane 6:63-69) 
15. Tiyenera Kukhala ndi Nzeru Yoyenera ya Choonadi (Yohane 6:60-71) 
 
Yesu Anatipatsa Moyo Osatha Kupitira mu Mnofu Wake ndi Magazi

M’pingo ukusunga masakalamenti awiri olamulidwa ndi Yesu. Oyamba ndi ubatizo, ndipo wina ndi Mgonero Oyera. Tikutengako mbali mu Mgonero kuti tilingalire pa Choonadi cha uthenga chovumvulutsidwa mu mkate wake ndi mu vinyo, mwa kukumbukira uthengau.
Mu chiphikiro cha Mgonero Oyera, tikudya mkate mwa kukhumbukira mnofu wa Yesu, ndipo tikumwa vinyo ngati chiphikiro cha magazi Ake. mwakutero, tanthauzo lenileni la Mgonero Oyera ndi kulimbikitsa chikhulupiliro chathu mu Choonadi chakuti Yesu anatipulumutsa kumachimo adziko ndipo anatipatsa moyo osatha kupitira mu ubatizo Wake ndi imfa Yake pa Mtanda.
Koma, bvuto ndi lakuti pafupi-fupi Akristu onse akutengako mbali mu Mgonero Oyera mwachizolowezi, kopanda ngakhalenso kuzindikira cimene Yesu anatanthauza ndi mawu, “Mnofu Wanga ndi chakudwadi, ndipo magazi Anga ndi chakumwa chenicehni” (Yohane 6:55). Chotero, mkati mwa uthenga wa madzi ndi Mzimu, tikuyenera kulingaliranso pa tanthauzo la Yesu kutilamula kuti tidye mnofu Wake ndi kumwa magazi Ake, ndi kukhulupilira m’menemo.
Thêm

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?