Search

SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Phúc-âm Giăng

Tiếng Chichewa  19

Ziphunzitso pa Uthenga wa Yohane (Ⅱ) - Chikondi cha Mulungu Chovumbulutsidwa Kupitira mwa Yesu, Mwana Wobadwa Yekha (Ⅱ)

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928239757 | Trang 0

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkatimu

Kulambulabwalo 

CHAPITALA 3
1. Tiyenera Kubadwa Mwatsopano Mwa Kukhulupilira mu Uthenga wa Madzi ndi Mzimu (Yohane 3:1-15) 
2. Ambuye Athu Anabwera Padzikoli Kudzatipulumutsa Kumachimo Adziko (Yohane 3:14-21) 
3. Kodi Tiyenara Kukhulupilira M’chiyani Pamaso pa Mulungu? (Yohane 3:21) 
4. Mulungu Wathu Ndiye Ambuye Amene Anatipatsa Umoyo Wosatha, Woona (Yohane 3:35-36) 

CHAPITALA 4
1. Ambuye Amene Amathetsa Mabvuto Athu onse (Yohane 4:3-19) 
2. Kodi Ndi M’chiyani M’mene Mitima Yathu Ikupeza Chikhutilitso? (Yohane 4:10-24) 
3. Madzi Amoyo Amene Amapangitsa Munthu Kuti Asamvenso Ludzu (Yohane 4:13-26, John 4:39-42) 
4. Kodi N’mtundu Otani wa Chikhulupiliro Umene Tifunika wa Chitsitsimutso Chathu cha Uzimu? (Yohane 4:19-26)
5. Mawu a Yesu Ndi Mawu a Mulungu (Yohane 4:46-54) 

CHAPITALA 5
1. Sitiyenera Kubwereranso Ku Chiyuda (Yohane 5:10-29) 
2. Ambuye Ayendera Dziwe la ku Betiseda (Yohane 5:1-9) 

CHAPITALA 6
1. Gwirani Nchito ya Kuti Mpeze Chakudya Chokhalitsa Chopeleka Moyo Wosatha (Yohane 6:16-40) 
 
Chikodi Chovumbulutsidwa Kupitira mwa Yesu Khristu

Chinalembedwa, “Palibe munthu anaonapo Mulungu ndi kale lonse, Mulungu wobadwa yekha amene ali pachifuwa cha Atate ndiye amene anafotokoza za Mulungu” (Yohane 1:18).
Yesu anaulura mokwana bwanji chikondi cha Mulungu kwaife! Kodi ndi choona cheni-cheni chotani chachipulumutso chili mu uthenga wa madzi ndi Mzimu! Sitinadzitsutse polandira chipulumutso kupitira mu chikhulupiliro chathu mwa Yesu, amene anabwera mwa madzi ndi magazi. (1 Yohane 5:6).
Ndikhulupilira kuti nonsenu m’kukhulupilira mwa Yesu Khristu amene anavumbulutsa chikondi cha Mulungu, sungani chikhulupiliro mu chikondi Chake m’mitima yanu, ndipo nthawi zonse mkhale ndi moyo pacifukwa cha kufalitsa chikondicho. Ndikhulupilira kuti mdzafuna dalitso la chikhulukiro cha uchimo mwa kukumana ndi Mulungu kupitira mu uthenga wa madzi ndi Mzimu.
Thêm

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?