Search

SÁCH ĐIỆN TỬ VÀ SÁCH NÓI MIỄN PHÍ

Phúc-âm theo Ma-thi-ơ

Tiếng Chichewa  13

ULALIKI PA UTHENGA WABWINO WA MATEYU (II) - KODI TINAKHULUPIRIRA CHIYANI KUTI TILANDIRE CHIKHULULUKIRO CHA MACHIMO?

Rev. Paul C. Jong | ISBN 9788928260089 | Trang 512

Tải xuống sách điện tử và sách nói MIỄN PHÍ

Chọn định dạng tệp ưa thích và tải xuống an toàn vào điện thoại di động, máy tính hoặc máy tính bảng để đọc và nghe các bộ sưu tập bài giảng mọi lúc mọi nơi. Tất cả sách điện tử và sách nói đều hoàn toàn miễn phí.

Bạn có thể nghe sách nói qua trình phát bên dưới. 🔻
Sở hữu sách in
Mua sách in trên Amazon
Zamkatimu 
 
Mau Oyamba 

MUTU 9
1. Khulupilirani mwa Yesu Kristu Yemwe Anadza Monga Mulungu Wathu (Mateyu 9:1-13) 
2 .Yesu Yemwe Anadza Kudzapulumutsa Ife, Amanjenje Auzimu (Mateyu 9:1-13) 
3. Chikhulupiliro cha Chipembedzo Motsutsana ndi Chikhulupiliro mu Mphamvu ya Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu (Mateyu 9:1-13) 
4. Antchito a Mulungu (Mateyu 9:35-38) 

MUTU 10
1. Mphamvu Yochiritsa Matenda Onse Imapezeka mu Uthenga Wabwino wa Madzi Ndi Mzimu (Mateyu 10:1-16) 
2. Tiyeni Tikhale Monga Antchito a Mulungu (Mateyu 10:1-8) 

MUTU 11
1. Yohane Mbatizi Sanali Wolephera (Mateyu 11:1-14) 

MUTU 12
1. Yesu Ananena Kuti Iye Amafuna Chifundo Osati Nsembe (Mateyu 12:1-8) 
2. Kodi Mukufuna Kudziwa Kuti Kuchitira Mwano Mzimu Woyera ndi Chiani? (Mateyu 12:9-37) 
3. Tchimo Losakhululukidwa komaso Ntchito ya Obadwa Mwatsopano (Mateyu 12:31-32)
4. Kodi Satana Amafuna Kukhala Kuti? (Mateyu 12:43-50) 

MUTU 13 
1. Fanizo la Mitundu Inayi ya Minda (Mateyu 13:1-9) 
2. Inu Mwaloledwa Kudziwa Zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba (Mateyu 13:10-23) 
3. Ufumu wa Kumwamba Ufanizidwa ndi Munthu, Amene Anafesa Mbeu Zabwino M’munda Mwace (Mateyu 13:24-30) 
4. Mphamvu ya Uthenga Wabwino wa Madzi ndi Mzimu (Mateyu 13:31-43) 
5. Ufumu wa Kumwamba Uli Wofanana ndi Cuma Cobisika M’munda (Mateyu 13:44-46)
6. Ufumu wa Kumwamba Uli Wofanana ndi Khoka Loponyedwa m’Nyanja Ndi Kusonkhanitsa Pamodzi Za Mitundu Yonse (Mateyu 13:47-52) 
7. Mariya Ndithudi Si Waumulungu (Mateyu 13:53-58)
 
Mtumwi Mateyu akutiuza ife kuti Mau a Yesu analankhulidwa kwa aliyense m’dziko lino, popeza Iye ankaona Yesu monga Mfumu ya mafumu. Tsopano, Akristu dziko lonse lapansi, amene angobadwa mwatsopano pokhulupilira mu uthenga wabwino wa madzi ndi Mzimu omwe tikufalitsa, indedi akufunitsitsa kudya mkate wamoyo. Koma ndikobvuta kwa iwo kukhala ndi chiyanjano ndi ife mu uthenga wabwino weni weni, popeza iwo onse ali kutali ndi ife. Choncho, kuti tikumane ndi zofunika zauzimu za anthu amenewa a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ulaliki m’buku limeneli wakonzedwa monga mkate watsopano wa moyo kwa iwo kuti usamalire kukula kwao kwauzimu. Mlembi amanena kuti iwo amene alandira chikhululukiro cha machimo ao pokhulupilira m’Mau a Yesu Kristu, Mfumu ya mafumu, ayenera kudya Mau Ake angwiro pofuna kuteteza chikhulupiliro chao komanso kuchita bwino m’miyoyo yao yauzimu. Buku limeneli lidzapereka mkate weni weni wamoyo wauzimu kwa inu nonse amene mwakhala anthu olemekezeka a Mfumu mwa chikhulupiliro. Kudzera mu Mpingo Wake ndi akapolo Ake, Mulungu adzapitiriza kupereka kwa inu mkate umenewu wamoyo. Lolani madalitso a Mulungu akhale pa inu nonse amene mwabadwa mwatsopano mwa madzi ndi Mzimu, amene mukufuna kukhala ndi chiayanjano chauzimu ndi ife mwa Yesu Kristu.
Thêm
Sách In Miễn phí
Thêm sách in vào giỏ
Trình phát sách nói

Những sách liên quan đến tựa đề này

The New Life Mission

Tham gia khảo sát của chúng tôi

Bạn biết đến chúng tôi qua đâu?